Professional Documents
Culture Documents
Book of Ephesians
Book of Ephesians
oyera mtima amene ali m'Efeso, ndi kwa iwo okhulupirika mwa Khristu Yesu: 2
Chisomo kwa inu, ndi mtendere wochokera kwa Mulungu Atate wathu, ndi
Ambuye Yesu Khristu.
Khristu, amene anatidalitsa ife ndi dalitso lonse la mzimu m'zakumwamba mwa
Khristu; 4 Aro. 8.28; Akol. 1.22; 1Pet. 1.2, 20 monga anatisankha ife mwa Iye,
lisanakhazikike dziko lapansi, tikhale ife oyera mtima, ndi opanda chilema pamaso
pake m'chikondi. 5 Aro. 8.29-30; Agal. 4.5 Anatikonzeratu tilandiridwe ngati ana
a Iye yekha mwa Yesu Khristu, monga umo kunakomera chifuniro chake, 6 Aro.
3.24 kuti uyamikidwe ulemerero wa chisomo chake, chimene anatichitira ife
kwaufulu mwa Wokondedwayo. 7 Aro. 2.4; Akol. 1.14 Tili ndi maomboledwe
mwa mwazi wake, chikhululukiro cha zochimwa, monga mwa kulemera kwa
chisomo chake, 8chimene anatichulukitsira ife m'nzeru zonse, ndi
chisamaliro. 9 Akol. 1.26 Anatizindikiritsa ife chinsinsi cha chifuniro chake,
monga kunamkomera ndi monga anatsimikiza mtima kale mwa Iye, 10 Agal. 4.4;
Aef. 2.15; Afi. 2.9-10 kuti pa makonzedwe a makwaniridwe a nyengozo,
tinakonzekeratu monga mwa chitsimikizo mtima cha Iye wakuchita zonse monga
mwa uphungu wa chifuniro chake; 12 Aef. 1.6, 14 kuti ife amene tinakhulupirira
Khristu kale tikayamikitse ulemerero wake. 13 Yoh. 1.17; Aef. 4.30 Mwa Iyeyo
ulamuliro, ndi mphamvu, ndi ufumu, ndi dzina lililonse lotchedwa, si m'nyengo
yino ya pansi pano yokha, komanso mwa iyo ikudza; 22 Mas. 8.6; Akol.
1.18 ndipo anakonza zonse pansi pa mapazi ake, nampatsa Iye akhale mutu pamtu
pa zonse, kwa Mpingo 23 Akol. 1.18; 2.14, 20 amene ali thupi lake, mdzazidwe
Aefeso 2
ndi kuchita zifuniro za thupi, ndi za maganizo, ndipo tinali ana a mkwiyo
chibadwire, monganso otsalawo; 4 Aef. 2.7; Aro. 2.4 koma Mulungu, wolemera
choposa cha chisomo chake, m'kukoma mtima kwa pa ife mwa Khristu
Yesu. 8 Yoh. 6.65; Aro. 3.24; 4.16 Pakuti muli opulumutsidwa ndi chisomo
chakuchita mwa chikhulupiriro, ndipo ichi chosachokera kwa inu: chili mphatso ya
Mulungu; 9 Aro. 3.20, 28 chosachokera kuntchito, kuti asadzitamandire munthu
aliyense. 10 1Ako. 3.9; 2Ako. 5.5, 17 Pakuti ife ndife chipango chake, olengedwa
mwa Khristu Yesu, kuchita ntchito zabwino, zimene Mulungu anazipangiratu, kuti
tikayende m'menemo.
Ayuda ndi amitundu ayanjanitsidwa ndi Mulungu mwa mtanda wa Khristu
11 Akol. 1.21 Momwemo kumbukirani, kuti kale inu amitundu m'thupi,
Khristu, alendo a padera ndi mbumba ya Israele, ndi alendo alibe kanthu ndi
mapangano a malonjezano, opanda chiyembekezo, ndi opanda Mulungu m'dziko
lapansi. 13 Yes. 57.19; Mac. 2.39 Koma tsopano mwa Khristu Yesu inu amene
munali kutali kale, anakusendezani mukhale pafupi m'mwazi wa Khristu. 14 Mik.
5.5 Pakuti Iye ndiye mtendere wathu, amene anachita kuti onse awiri akhale
mmodzi, nagumula khoma lakudulitsa pakati, 15 Akol. 2.14, 20 atachotsa udani
m'thupi lake, ndiwo mau a chilamulo cha kutchulako malangizo; kuti alenge
awiriwa mwa Iye yekha, akhale munthu mmodzi watsopano, ndi kuchitapo
mtendere; 16 Akol. 1.20-22 ndi kuti akayanjanitse awiriwa ndi Mulungu, m'thupi
limodzi mwa mtandawo, atapha nao udaniwo; 17 Yes. 57.19; Mac. 2.39 ndipo
m'mene anadza, analalikira Uthenga Wabwino wa mtendere kwa inu akutali, ndi
mtendere kwa iwo apafupi; 18 Yoh. 14.6 kuti mwa Iye ife tonse awiri tili nao
malowedwe athu kwa Atate, mwa Mzimu mmodzi. 19 Afi. 3.20 Pamenepo ndipo
simulinso alendo ndi ogonera, komatu muli a mudzi womwewo wa oyera mtima
ndi a banja la Mulungu; 20 Mat. 16.18; 21.42 omangika pa maziko a atumwindi
aneneri, pali Khristu Yesu mwini, mwala wa pangodya; 21 1Ako. 3.17; Aef. 4.15-
16 mwa Iye chimango chonse cholumikizika pamodzi bwino, chikula, chikhale
Kachisi wopatulika mwa Ambuye; 22 1Pet. 2.5 chimene inunso mumangidwamo
Aefeso 3
Chinsinsi cha maitanidwe a amitundu
1 Mac. 21.33 Chifukwa cha ichi ine Paulo, ndine wandende
wa KhristuYesu chifukwa cha inu amitundu, 2 Mac. 9.15 ngatitu munamva za
udindo wa chisomo cha Mulungu chimene anandipatsa ine cha kwa inu; 3 Agal.
1.12; Akol. 1.26-27 ndi umo anandizindikiritsa chinsinsicho mwa vumbulutso,
ziwalo zinzathu za thupilo, ndi olandira nafe pamodzi palonjezano mwa Khristu
Yesu, mwa Uthenga Wabwino, 7 Akol. 1.23, 25 umene anandikhalitsa mtumiki
wake monga mwa mphatso ya chisomo cha Mulungu, chimene anandipatsa ine,
monga mwa machitidwe a mphamvu yake. 8 1Ako. 15.9 Kwa ine wochepa ndi
akhale chikhalire mwa chikhulupiriro m'mitima yanu; kuti, ozika mizu ndi
otsendereka m'chikondi, 18 Aef. 1.18 mukakhozetu kuzindikira pamodzi ndi oyera
mtima onse, kupingasa, ndi utali, ndi kukwera, 19 Akol. 2.9-10 ndi kuzama
Aefeso 4
Mulungu, chifukwa cha chipulukiro chili mwa iwo, chifukwa cha kuumitsa kwa
mitima yao; 19 Aro. 1.24, 26 amenewo popeza sazindikiranso kanthu konse,
ntchito, nagwire ntchito yokoma ndi manja ake, kuti akhale nacho chakuchereza
wosowa. 29 Akol. 3.8, 16 Nkhani yonse yovunda isatuluke m'kamwa mwanu,
koma ngati pali ina yabwino kukumangirira monga mofunika ndiyo, kuti ipatse
chisomo kwa iwo akumva. 30 Yes. 63.10; Aef. 1.13 Ndipo musamvetse chisoni
mtima, ndi mkwiyo, ndi chiwawa, ndi mwano zichotsedwe kwa inu, ndiponso
choipa chonse. 32 Mrk. 11.25; 1Pet. 3.8-9 Koma mukhalirane okoma wina ndi
Aefeso 5
monga ana a kuunika, 9pakuti chipatso cha kuunika tichipeza m'ubwino wonse, ndi
chilungamo, ndi choonadi, 10kuyesera chokondweretsa Ambuye
nchiyani; 11 1Ako. 5.9, 11; 10.20 ndipo musayanjane nazo ntchito za mdima
zosabala kanthu, koma makamakanso muzitsutse; 12 Aro. 1.24, 26 pakuti
zochitidwa nao m'tseri, kungakhale kuzinena kuchititsa manyazi. 13 Yoh. 3.20-
21 Koma zinthu zonse potsutsika ndi kuunika, zionekera; pakuti chonse
chakuonetsa chili kuunika. 14 Yes. 60.1; Aro. 6.4-5; 13.11-12 Mwa ichi anena,
Khala maso wogona iwe, nuuke kwa akufa, ndipo Khristu adzawala pa iwe.
15 Akol. 4.5 Potero, penyani bwino umo muyendera, si monga opanda nzeru,
koma monga anzeru; 16akuchita machawi, popeza masiku ali oipa. 17 1Ate.
4.3 Chifukwa chake musakhale opusa, koma dziwitsani chifuniro cha Ambuye
nchiyani. 18 Miy. 20.1; Luk. 21.34 Ndipo musaledzere naye vinyo, m'mene muli
chitayiko; komatu mudzale naye Mzimu, 19 Mac. 16.25 ndi kudzilankhulira nokha
ndi masalmo, ndi mayamiko, ndi nyimbo zauzimu, kuimbira ndi kuimba
m'malimba Ambuye mumtima mwanu; 20 Mas. 34.1; Akol. 3.17 ndi kuyamika
Khristu.
22 Akol. 3.18 Akazi inu, mverani amuna anu a inu eni, monga kumvera
Ambuye. 23 1Ako. 11.3 Pakuti mwamuna ndiye mutu wa mkazi, monganso
azisiya atate ndi amai, nadzaphatikizana ndi mkazi wake; ndipo iwo awiri
adzakhala thupi limodzi. 32Chinsinsi ichi nchachikulu; koma ndinena ine za
Khristu ndi Mpingo. 33 1Pet. 3.6 Komanso inu, yense pa yekha, yense akonde
mkazi wake wa iye yekha, monga adzikonda yekha; ndipo mkaziyo akumbukire
kuti aziopa mwamuna.
Aefeso 6
1 Miy. 23.22; Akol. 3.20 Ananu, mverani akukubalani mwa Ambuye, pakuti
ichi nchabwino. 2 Eks. 20.12 Lemekeza atate wako ndi amai ako (ndilo lamulo
loyamba lokhala nalo lonjezano), 3kuti kukhale bwino ndi iwe, ndi kuti ukhale wa
nthawi yaikulu padziko. 4 Deut. 6.7, 20, 24; Akol. 3.21 Ndipo atate inu,
musakwiyitse ana anu; komatu muwalere iwo m'maleredwe ndi chilangizo cha
Ambuye.
5 Akol. 3.22-24 Akapolo inu, mverani iwo amene ali ambuye anu monga mwa
thupi, ndi kuwaopa ndi kunthunthumira nao, ndi mtima wanu wosakumbukira
kanthu kena, monga kwa Khristu; 6 Akol. 3.22-24 si monga mwa ukapolo wa
kuwaopsa; podziwa kuti Ambuye wao ndi wanu ali m'Mwamba, ndipo palibe
tsankho kwa Iye.
Zida za Mulungu
10 Akol. 1.11 Chotsalira, tadzilimbikani mwa Ambuye, ndi m'kulimba kwa
mphamvu yake. 11 2Ako. 6.7 Tavalani zida zonse za Mulungu, kuti mudzakhoze
kuchilimika pokana machenjerero a mdierekezi. 12 Luk. 22.53; Aef. 2.2 Chifukwa
kuti kulimbana kwathu sitilimbana nao mwazi ndi thupi, komatu nao maukulu, ndi
maulamuliro, ndi akuchita zolimbika a dziko lapansi a mdima uno, ndi auzimu a
choipa m'zakumwamba. 13 2Ako. 10.4 Mwa ichi mudzitengere zida zonse za
Mulungu, kuti mudzakhoza kuima chitsutsire pofika tsiku loipa, ndipo, mutachita
zonse, mudzachilimika. 14 Yes. 11.5; 59.17 Chifukwa chake chilimikani,