Professional Documents
Culture Documents
Treasa Cinyanja
Treasa Cinyanja
Treasa Cinyanja
2022 -2024
Grade 10,11, 12 & GCE
QUESTIONS
AND
MFUGULO
Nkhoma T.
ONANI ANGONI (K.D. Philip)
25 Chulani miko atatu amu Africa kumene kupezeka angoni masiku ano.
26 Lembani mwacidule nkhani zimene zipezeka m’buku la onani angoni.
MFUGULO
ONANI ANGONI (K.D.Philip)
1 Chaka Zulu
2 Zungendawa
3 Angoni atafika pa Zambezi anapeza munthu woolotsa anthu ndi boti ndipo mfumu
anamupempha munthuyo kuti awawo lotse. Pamene onse anatha kuoloka, anamgwira
munthuyo woolotsa namupha kuopa kuti angadzawolotserenso adani.
4 Mwana wamfumu woyamba kubadwa makamaka wamwamuna.
5 – Kubvala zikumba
- Kudoola makutu
- Cilankhulo cao
- Zakudya zao
6 Angoni amaonetsa ulemu polandila ndi popereka, kuitana ndi kubvomera, ulemu wa
Malo. Ngati amfumu akhala pa mupando ena onse akhala pansi. Pakudya ayamba ndi
akulu.
8 Angoni anacoka ku south Africa cifukwa ca nkhondo ya chaka ndi kucepa kwa malo.
(iii) Mputa anacoka pamodzi ndi gulu la Mzilikazi kulowera kumpoto panjira ku
Transvaal anakangana ndipo gulu la mputa linapitirira ndi ulendo wao kuoloka
Zambezi ku mbali ya Tete ku lowa mu Mozambique. Anapitirira ndi ulendo
wawao kufika mu dziko la Malawi ku Domwe pafpi ndi boma la Dedza. Atamva
za mbiri ya angoni a zungendawa wochedwanso Magwambani anacoka pa
Domwe nalowa mdziko la Malawi ku mwera kwa Dedza ku Ncheu. Atasautsa ndi
nkhondo yake anaoloka m’tsinje washire ku fika ku Tanzania ku malo ochedwa
Mngongomwa (matengo). Anakomana ndi gulu la Zulu Gama a gulu la
Zungendawa. Anamenyana ndipo Mputa anapambana nakhala mfumu. Atakhala
mfumu kwa nthaw yaitali, Angoni a Zulugama anaukira gulu la mputa, mputa
anaphedwa ndipo pamene pa mene panathera gulu la mputa.
(iii) Fundanimphasa
13 kuthira nsembe ndiko kuononga cinthu cina ca moyo kapena copanda moyo cifukwa
-
Anali kuthira nsembe ngati m’banja mwaoneka zobvuta monga maliro, nthenda
ndi matsoka.
- Ngati m’modzi wa banja alota aliula nkhula ndi umodzi wa banja amene anafa
kale.
- Munthu anafa kale ali kupempha kanth kena.
14 Amaloola, kutenga Cuma ca ziweto kapena ndalama ndikupereka ku banja la makolo a
mkazi.
15 (i) - lihawo
- mkondo
- mbemba
- mpeni
(ii) Mpeni waung’ono unali wocotsera minga kapena cida pa thupi ngati umodzi
walasidwa ndi mdani.
17 Anali kupha anthu ambiri ndi ziweto kuti akhale msamiro ndinso kuti anthu adye pa
maliro.
- kuphunzitsa ana amuna ndodo kuti akhale ocenjera ndi olimba mtima pa
kumenyana.
20 Anali kupinda maondo amunthu wakufayo ndi kummangirira mcikopa kapena nsalu
atammanga conco anali kumkhazika cansonga pamodzi ndi zida zake.
Anali kucita tero cifukwa anali kukhulupirira kuti msirikari wa nkhondo sagona.
21 Mau akuti ‘kuutha’ atanthauza kukonza pena kumanga kwake kwa maliro.
22 kulankhula mau oipa, kuonga zinthu za eni dala pena mwa ngozi
23 wogwidwa cigololo anali kuphedwa. Wogwidwa ufiti nayenso anali kupedwa ndi