Professional Documents
Culture Documents
English
English
PEPALA LACHIWIRI
(Malikisi 50)
Malangizo
2
3. Yankhani mafunso onse mu gawo A, B ndi C.
3
4
4. Onetsani funso lililonse lomwe mwayankha pochonga mu
kabokosi kali ku tsogoloko. 5
KUMVETSA NKHANI
TSOKA LA SELINA
3
NAME __________________________________________ SCHOOL _______________________
i. Wandigwiritsa chikho mkati
________________________________________________________________
________________________________________________________________
________________________________________________________________
(malikisi 3)
________________________________________________________________
________________________________________________________________
(malikisi 2)
4
NAME __________________________________________ SCHOOL _______________________
i. Selina akadachita chani kuti apewe mavuto onse omwe adakumana
nawo?
________________________________________________________________
________________________________________________________________
(Malikisi 2)
j. Perekani ufulu uwiri omwe ophunzira amakhala nawo
________________________________________________________________
________________________________________________________________
(malikisi 2)
Anthu onse pasiwa paja adali khumakhuma podziwa kuti tsikulo silitha
bwino. Atsibweni a Ndagona adaonetseratu kuti adali wokwiya kwambiri
ndi khalidwe la mpongozi wawo. Anthuwo adali maso yuu kunjira
kudikirira Mfumu Zathaizi yomwe inabwera kudzaonerera mwambo wosudzula
amake Ndaipalero, mkazi wa Ndagona.
5
NAME __________________________________________ SCHOOL _______________________
anthu adakhulupirira zonena za mwanayu ndipo adangoti adzaona pakuti
amake Ndaipalero adawachenjerera pogona.
Anthu akumudziwo sadadziwe kuti chifukwa chenicheni chimene
Chodziwadziwa adachokera kutawuni chidali chakuti iye ankathawa
apolisi.Chidachitika chidali chakuti, tsiku lina Chodziwadziwa ndi
anzake asanu adapita kukayenda ku masitolo a kutauni kuja. Ali
chiyendere, adakumana ndi ana a amwenye atatu amene adali kudya zakudya
zosiyanasiyana. Chodziwadziwa ndi anzake aja adalephera kuugwira mtima
ndipo adatsomphola zakudya zija n’kuvulaza mmodzi mwa ana a amwenyewo.
Kholo la mwanayo lidaimba lamya ku polisi ndipo posachedwa apolisi
adali nyomi pambuyo pa tiakapsala tija. Mwayi wa Chodziwadziwa udali
woti sadagwidwe, anzake onse aja adawakwidzinga unyolo.
Usiku watsiku limenelo Chodziwadziwa adalongeza katundu wake
natulukira pazenera, naubutsa wa kumudzi. Atafunsidwa kumudzi chomwe
adachokera kutawuni, iye adangotchula pavunda khola. Iye adanama kuti
wathawa nkhanza za amake Ndaipalero.
Mfumu Zathaizi idafika dzuwa likuswa mtengo. Iyo idabwera ndi nduna
ziwiri. Mfunseni, nduna Yachiwiri, adayamba kuyankhula, “Mosataya
nthawi tipemphe mkokowogona wakuchimuna kuti usudzule amake
Ndaipalero, zikomo”
“Ife, mfumu, tilibe mtunda wautali.” Mwatipeza adafotokoza. “Titakhala
pansi pamudzi pano tagwirizana kuti amake Ndaipalero ndi ana awo
abwerere kwawo pakuti mnzawo amene adawabweretsa kunoyo watsamira
mkono. Tiwasudzula ndi K50 iyi. Ndikatero ndaima. Mukafunsa za chuma
cha Ndagona, mayiyu ndi ana akewo satengapo kanthu. Iwowa zawo
adadyeratu wathu ali moyo.
6
NAME __________________________________________ SCHOOL _______________________
zomwe adakuuzani Chodziwadziwa. Komatu leroleroli apolisi adali
kunyumba kwanga ndipo andiuza chifukwa chenicheni chimene nthyamba
wanuyu adachokera kutawuni. Si chifukwa cha amake Ndaipalero ayi, koma
chifukwa cha magwiragwira a mwana wanuyu! ndiye ine mfumu Zathaizi,
ndikuti chumachi ati atenge ndi mayiyu ndi ana ake. Inu yanu ikhala
nyumba yokhayi pakuti ili pamudzi panu. Igwani apa ndi…..”
Mfumu Zathaizi sidatsirize mawu ake, pakuti apolisi adangoti
balamunthu kutulukira. Chodziwadziwa adati ayesere kuthawa koma agalu
apolisi adamuwakha. Manyazi, mantha ndi chisoni zidawagwira anthu a
pamudzi paja. Adayamba kuchoka mmodzimmodzi, mitu ili werawera, manja
ali mkhosi.
7
NAME __________________________________________ SCHOOL _______________________
f. Tchulani chifukwa chimodzi zomwe Mfumu Zathaizi adapereka kuti
ateteze katundu wa amake Ndaipalero ndi ana awo.
________________________________________________________________
(Malikisi 1)
g. Tsimikizani mfundo yakuti ‘zakumva zipweteketsa mutu’ malinga ndi
nkhaniyi.
________________________________________________________________
_______________________________________________________________
(Malikisi 1)
3. Werengani ndakatulo ili m’munsiyi ndipo muyankhe mafunso
otsatirawo.
8
NAME __________________________________________ SCHOOL _______________________
Iyenda nibangula vuu!
Chamva ludzu achipatsa madzi
Kodi ichochi n`chamoyo?
Hii muli anthu mkatimo
Mzeru ya anthu njododometsa
9
NAME __________________________________________ SCHOOL _______________________
e. Perekani zipangizo zina ziwiri za nkhani zamchezo ndi
zolembedwa zomwe mlembi wafewetsera luso lake kupatula
zatchulidwa mu funso d.
___________________________________________________________
___________________________________________________________
(malikisi 2)
f. Tsindikani mwambi wakuti, ‘kusadziwa n’kufa komwe’
molingana ndi ndakatuloyi.
___________________________________________________________
___________________________________________________________
(malikisi 2)
________________________________________________________________
10
NAME __________________________________________ SCHOOL _______________________
________________________________________________________________
________________________________________________________________
________________________________________________________________
________________________________________________________________
________________________________________________________________
________________________________________________________________
________________________________________________________________
________________________________________________________________
________________________________________________________________
(malikisi 5)
(malikisi5)
11