Chichewa

You might also like

Download as pdf or txt
Download as pdf or txt
You are on page 1of 46

2024 SONGANI ZONE STD 8 MOCK EXAMINATIONS

CHICHEWA
(100 MARKS)
Dzina la ophunzira: _______________________________________________________________________
(Yambani la bambo)

Dzina la sukulu: _________________________________________________________________________


Malangizo
 Lembani dzina lanu komanso dzina la sukulu yanu
 Yankhani mafunso mosamalitsa
 Siyani kulemba komanso Perekani pepala lanu kwa oyang’anira mayeso mukafunsidwa kutero.

GAWO A
Yankahani funso limodzi lokha mwa mafunso awiri omwe ali m’musiwa. Sankhani mutu wa chimangirizo kapena
kalata.

Mawu achimangirizo chanu kapena kalata yanu asachepere 100 komanso asabzole 150.

1. Lembani chimangirizo pa mutu uwu moto olusa. Mwazina tsatani izi polemba.

Ndime yoyamba
 Tsiku ndi nthawi yomwe moto udabuka.
 Chomwe chidayambitsa moto.
 Malo omwe kudabuka moto.

Ndime yachiwiri
 Dera lomwe motowu udawononga.
 Zinthu zomwe zidawonongeka ndi motowu.

Ndime yachitatu.
 Gawo lomwe mudatenga patsikuli.
 Thandizo lomwe likufunika mwansanga.

KAPENA
2. Lembani kalata kwa mkulu owona zamaphunziro m’dera lanu yomufotokozera za mavuto omwe
mukukumana nawo pa sukulu yanu. Mwazina tsatani izi polemba.

Ndime yoyamba
 Cholinga cha kalata
 Dzina la sukulu yanu
 Chiwerengero cha ana pasukulupo
Ndime yachiwiri
 Mavuto omwe mukukumana nawo.
 Zomwe mukufuna atakuthandizani mwansanga

Ndime yachitatu
 Chisangalalo chanu mukadzalandira thandizolo.
 Momwe muzadsamalire katunduyo.
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
___________________________________________________________________________________________
GAWO B. (20 MALIKSI)

3. Werengani nkahni yotsatirayi mosamala kwambiri kenako yankhani mafunso otsatirawo.

Pabwalo pamakhala kanenedwe kake ka milandu kamene kamatchedwa chowa. Chowachi chimachitika pofuna
kuona bwino magwelo ake a milandu. Popeza kalero padalibe mchitidwe omalemba pamene oyankhula ali
kufotokoza. Oweluza adali kubwerezanso mawu aja amene munthu wanena. Tsopano uja ofotokoza amabuula
kuti mmm! mmm! Kuvomereza kuti obwereza mawu uja adali kulongosola molondola.

Pabwalo loweluzira milandu lotchedwa nkhani zathera pano, m’mawa tsiku loweluka dzuwa litangotuluka
pang’ono, anthu adali kudikira amfumu bwana Lumbe kuti ayambe kuweluza milandu. Mwadzidzidzi anthu
adaona mfumuyi ndi akulu abwalo, a Gudeya ndi a Muholo akutulukira kuti balamanthu. Anthu onse adangoti
gwadu gwadu. M’menemo nkuti Mbumulire pamtima pake pali thi thi thi. Mfumu bwana Lumbe adali ndi
chikaliwo wake chili ndi utsi kuti phwa, phwa phwa matsinya ali khwe, khwe, khwe ngati ayambana ndi munthu.

Ehe! Adayankhula mfumu bwana Lumbe akukhala pa chitsa cha mtengo. Nthawiyo akulu abwalo nkuti atakhala
kale pansi . “Chete!” adatero nkulu wa bwalo la nkhani zathera pano. Tsono mverani mfumu bwana Lumbe
“pano monga mudziwa,” adatero mfumu bwana Lumbe “ndi pankhani zathera pano pamene mboni zikupereka
umboni sindikufuna kumadzidula mawu. Pamene wina ali kufotokoza nkhani m’mene idayendera musamaikire
mang’ombe. Pomaliza nkhani iliyonse ndizagamula molingana ndi umboni ndi kakhalidwe ka nkhani.

Tsopano yankhani mafunso otsatirawa pa mizere iri pansi pa funso lililonse.

a. Kodi chowa ndi chiyani?


____________________________________________________________________________(Maliksi 1)
b. Kodi cholinga chochitira chowa ndi chiyani?
_____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________(Malikisi 2)
c. Chifukwa chiyani oweluza milandu akale adali kubwerezanso zomwe anthu anena
_____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________(2 Malikisi)
d. Fotokozani chifukwa chomwe ofotokoza milandu amabuulira.
_____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________(2 Maliksi)
e. Perekani matanthauzo a mawu awa kuchokera m’nkhaniyi.
(i). Balamanthu
____________________________________________________________________________(2 Malikisi)
(ii). Mang’ombe
____________________________________________________________________________(2 Malikisi)
f. Kodi mawu oti akulu abwalo akutanthauzanji?
_____________________________________________________________________________________
__________________________________________________________________________(2 Malikisi)
g. Perekani mivekero iwiri kuchokera mu nkhaniyi
___________________________________________________________________________(2 malikisi)
h. Perekani dzina la mfumu ikupezeka m’nkhaniyi.
____________________________________________________________________________(2 Malikisi)
i. Perekani malo omwe nkhaniyi idachitikira.
____________________________________________________________________________(1 Malikisi)
j. Perekani mutu wa nkhaniyi.
_____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________(2 Maliksi)
GAWO C.

4.Werengani kankhanika ndipo muyankhe mafunso otsatirawa.

“Ine maliro oterewa sindingaikitse.


Malemu agona apawa anadula phazi kale
kumudzi kuno”.

Mafunso

a. (i). Ndimalonje anji amenewa?


__________________________________________________________________________________(1 Maliksi)
(ii). Angalankhule malonjewa ndani?
__________________________________________________________________________________(1 Malikisi)
(iii). Mawu oti “adadula phazi” akutanthauzanji?
__________________________________________________________________________________(1Malikisi)

b. Kodi kuvula chipewa pamaso pa akuluakulu kumatanthauzanji?


__________________________________________________________________________________(1 Malikisi)
c. Perekani ntchito imodzi ya zikwangwani za pamsewu.
__________________________________________________________________________________(1 Malikisi)

5. Kupanga ziganizo

Pangani ziganizo zomveka bwino ndi mawu awa.

a. mtolankhani ______________________________________________________________________
b. mosamala ________________________________________________________________________
c. wokongola________________________________________________________________________
d. khu______________________________________________________________________________
e. ndiponso_________________________________________________________________________

GAWO D.
Mafunso 6 mpaka 10 sankhani mtundu wa mawu 10. Utsadutse pano palibe njira.
omwe atsekedwa mnzere kunsi kwawo mziganizo A. Mfotokozi dzina C. Mperekezi
zotsatirazi. B. Dzina D. Mneni

6. Khalidwe limeneli walitenga kuti? Mafunso 11 mpaka 15. Sankhani kanenedwe


A. Mfotokozi C. Mneni ka aneni ka ziganizo zotsatirazi.
B. Dzina D. Mlumikizi 11. Kodi mukulemba mayeso?
A. Kufunsa C. Kopempha
7. Ogo ine! Mphale ija yataika. B. Kolamula D. Kachifuniro
A. Mvekero C. Mperekezi
B. Mneni D. Mfuliro 12. Mutipatseko zovala zanuzo.
A. Kofotokoza C. Kopempha
8. Bwanji sunabwere? B. Kachifundo D. Kolamula
A. Mperekezi C. Muonjezi
B. Mneni D. Mlowammalo 13. Nyamuka uzipita pompano.
A. Kopempha C. Kofotokoza
9. Wandibera limene ndagula. B. Kolamula D. Kachifundo.
A. Mlowammalo C. Mfotokozi
B. Mneni D. Muonjezi 14. N’chiyani watengacho?
A. Kopempha C. Kolamula 25. Pasukulu panali _______ .
B. Kofunsa D. Kofotokoza. A. Ndwi C. Mbuu
B. Zi D. Phee
15. Chonde, ndimvereni chisoni.
A. Kachifuniro C. Kovomera Mafunso 26 mapaka 30. Sankhani mitundu
B. Kolamula D. Kufotokoza ya nsintho wa aneni m’ziganizo zotsatirazi.
26. Agalu alumana zedi.
Mafunso 16 mpaka 20 sankhani ntchito za
A. Wochititsa C. Wobwereza bwereza
aperekezi omwe atsekedwa mzere kunsi
B. Wochititsitsa D. Wochitirana
kwawo m’ziganizo zotsatirazi.
16. Agogo apita ku msika. 27. Nkhosa yagundidwa ndi njinga.
A. Kusonyeza umwini C. Kusonyeza nthawi A. Wochitidwa C. Wochitirana
B. Kusonyeza malo D. Kusonyeza mbali B. Wochititsa D. Wochititsitsa

17. Achimwene abwera nthawi ya madzulo. 28. Malita wabesa ndalama zonse.
A. Kusonyeza mbali C. Kusonyeza malo A. Wochitirana C. Wochitidwa
B. Kusonyeza chipangizo D. Kusonyeza ntahwi B. Wobwerezabwereza D. Wochititsa.

18. Nyumbayi ndi ya aNambewe. 29. Iye amadutsadutsa pano.


A. Kusonyeza m’gwirizano C. Kusonyeza A. Wochitirana C. Wobwerezabwereza
nthawi B. Wochititsa D. Wochititsitsa
B. Kusonyeza umwini D. Kusonyeza malo
30. Boma lapereka chimanga kwa anthu ovutika.
19. Yohane amumenya ndi mpini. A. Wochitirana C. Wochititsitsa
A. Kusonyeza nthawi C. Kusonyeza chipangizo B. Womchitira D. Wobwerezabwereza
B. Kusonyeza nthawi D.Kusonyeza malo
Mafunso 31 mpaka 35. Sankhani
20. Dzuwa limalowera ku madzulo. matanthauzo a mikuluwiko yotsatirayi.
A. Kusonyeza mbali C. Kusonyeza umwini
B. Kusonyeza nthawi D. Kusonyeza chipangizo. 31. Khoswe akakhala pa mkhate sapheka.
A. Mlandu ukakhala wako umaweluzika bwino
Mafunso 21 mpaka 25. Sankhani mvekero woyenera B. Mlandu wa m’bale umavuta kuweluza
kukhala mu m’pata uli mchiganizo chilichonse C. Mlandu ukakhalitsa umavuta kuweluza
mmusimu. D. Mlandu wa mfumu umaweluzika bwino.
21. Kumbuka anangoti __________ watulukira.
A. A. Vumbu C. Balamanthu 32. Fodya wako ndi uyo ali pamphuno wapachala
B. Mbwe D. Fwanthu. ngwamphepo.
A. Kudalira zinthu zomwe zili zako
22. Atate ali ___________ pakhonde. B. Kudalira zinthu zobwera
A. Mbuu C. Phe C. Kudalira zintu zopatsidwa
B. Ndwi D. Khuma D. Kudalira zintu zanzako, sibwino

23. Mbandayo idangoti ________ kusowa chonena. 33. Kuwongola mtengo mpoyamba.
A. Jenkha C. Yasa A. Kudulira mtengo usanakule kumapindulitsa
B. Phii D. Zi B. Ndi bwino kusamalira mtengo tchile
lisanakule
24. Anyamuka m’bandakucha kuli___________. C. Ndibwino kukonza zinthu zisanalakwikwe
A. Mbuu C. Psu D. Kukonza tsogolo ndi kwabwino kwambiri
B. Mbee D. Bi
34. Chikumbutsa nkhwangwa mchisanu.
A. Zinthu zina zimafunika panthawi yake. B. Kodi chimwemwe, wanyamula zingati.
B. Ntchito zina zinafunika kuthandizana. C. Kodi chimwemwe wanyamula zingati!
C. Ntchito zimafunika kuzigwira utakonzeka D. Kodi Chimwemwe wanyamula zingati?
D. Zinthu zina zimafunika nthawi zonse.
40. A. Yohane M’nyunga amakonda kuyimba
35. Mapanga awiri avumbwitsa. nyimbo.
A. Kuchita zinthu zambiri kumapindulitsa B. yohane m’myunga amakonda kuimba nyimbo?
B. Kuchita zinthu mofananitsa sikupindulitsa C. Yohane mnyunga amakonda kuimba nyimbo!
C. Kuchita zinthu ziwiri nthawi imodzi D. Yohane M’nyunga amakonda, kuimba
umapambana. nyimbo.
D. Kuchita zinthu ziwiri nthawi imodzi
sikupindulitsa. Mafunso 41 mpaka 45. Sankhani chachikazi cha
mawu omwe atsekedwa mzere kunsi kwawo
Mafunso 36 mpaka 40. Sankhani chiganizo mziganizo zotsatirazi.
chomwe chili ndi 41. Ndaona wafika ndi atatavyala ake.
zizindikirozamkalembedwe zoyenera A. Atengwa C. Amayi
m’ziganizo zotsatirazi. B. Apongozi D. Atate.

36. A. Amayi adati, “Choka iwe mwana wakuba”. 42. Fisi wagwira kachipsopsolo kaja.
B. amayi adati, “choka iwe mwana wakuba”. A. Kathazi C. Kamkota
C. Amayi adati. Choka iwe mwana wakuba. B. Kankhunda D. Kamsoti.
D. Amayi adati choka iwe mwana wakuba?
43. Nkhunzi ya agogo yathawa m’khola.
37. A. Aphunzitsi athu atenga kope pensulo ndi lula A. Msoti C. Msona
B. aphunzitsi athu atenga kope pensulo ndi lula. B. Nthoni D. Mkota
C. Aphunzitsi athu atenga kope, pensulo ndi lula.
D. Aphunzitsi athu atenga, kope, pensulo ndi 44. Mfumu yathu ndi yankhanza.
lula? A. Mfumakazi C. Mfumukazi
B. Ntchembere D. Mtenga
38. A. Mariya amayenda monyada?
B. Mariya amayenda monyada. 45. Talandira zambwe zinayi kochokera kwa a gogo.
C. maliya amayenda monyada! A. Nkhunda C. Nkhosa
D. maliya amayenda monyda. B. Mkota D. Mbuzi

39. A. Kodi Chimwemwe wanyamula zingati

MAFUNSO ATHERA APA


CHIRADZULU DISTRICT STANDARDISED EXAMINATIONS
2023 END OF TERM II EXAMINATION FOR STANDARD 7
CHICHEWA
(100 marks)

Dzina la Ophunzira: _______________________________________________________

GAWO A. (MALIKISI 30)


Langizo, yankhani funso limodzi lokha mwa mafunso ali mmunsiwa. Sankhani mutu wa chimangirizo kapena
wa Kalata. Mawu a chimangirizo chanu kapena kalata yanu asachepere 100 komaso asabzole 150.

1. Lembani chimangirizo pa mutu uwu; “MUDZI WATHU”


Mwazina, tsatani izi polemba chimangirizo chanu.

Ndime yoyamba
 Dzina la mudzi wanu
 Chigawo ndi boma komwe kuli mudzi wanu

Ndime yachiwiri
 Ena mwa magule omwe anthu amavina
 Zina mwa mbewu zomwe anthu amalima mmudzimo komanso nyama zomwe amaweta

Ndime yachitatu
 Ena mwa mavuto omwe anthu ammudzimo akukumana nawo ndi momwe mavutowo angathere

KAPENA
2. Mwamva kuti mwalephera mayeso a Sitandade 7 ndipo mukufuna kukabwerezera kwina.
Lembani kalata yopempha kwa mphunzitsi wamkulu wa ku Mchizeni Pulayimale Sukulu,
P.o. Box 10, Lisazi.
Mwazina tsatani izi polemba

Ndime yoyamba
 Ndinu mnyamata kapena nsungwana
 Muli ndi zaka zingati
 Munkaphunzira kuti

Ndime yachiwiri
 Zifukwa zitatu zomwe zakuchitisani kuti mufunsire malo ku sukuluyi
 Momwe mungalimbikirire malo atapezeka
Ndime yachitatu
 Mayina ndi makeyala awiri omwe angachitire umboni za inu

©CZ2023 Page 1 of 7
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________
___________________________________________________________________

©CZ2023 Page 2 of 7
GAWO B (Malikisi 20)

KUMVETSA NKHANI

3. Werengani nkhani yotsatirayi mosamala kwambiri kenaka Yankhani mafunso otsatirawo

A Patheratu atakambirana ndi makolo a Magireti adagwirizana zomuvomera kamwanje. Tsiku lotula mbeta kapena
la unkhoswe litakwana padaphedwa mbuzi ndi nkhuku zambiri. Padaphikidwanso thobwa lambiri. Padabwera anthu
ambiri akuchimuna komanso akuchikazi. Amayi akuchikazi ndi akuchimuna adatangwanidwa kuphika, thungululu
ndi ndi nyimbo za ukwati zidali mkamwa. Amuna adabindikira mkanyumba komata, kuthetsana malovu mkamwa
kukambirana nkhani za chiwongo ndi tsiku lomangitsa ukwati uku akumwa thobwa ndi kusinthana miphika ya
nkhuku. Nkhoswe yakuchikazi idali Teputepu pamene yakuchimuna idali Limbani.

Tsopano yankhani mafunso otastirawo

a. Kodi Patheretu adali yani?


_____________________________________________________________________________ (Malikisi 2)

b. Tchulani zinthu ziwiri zomwe amayi adatangwanika nazo.


_____________________________________________________________________________ (Malikisi 4)

c. Kodi nkhoswe yakuchikazi idali yani?


_____________________________________________________________________________ (Malikisi 2)
d. Perekani matanthauzo a mawu awa:
(i) M’kanyumba komata______________________________________________________ (Malikisi 2)
(ii) Tula mbeta _____________________________________________________________ (Malikisi 2)
(iii) Kuthetsana malovu mkamwa ________________________________________________ (Malikisi 2)

e. Perekani chimodzi cha mawu awa:


(i) Miphika _________________________________________________________________ (Malikisi 2)
(ii) Malovu _________________________________________________________________ (Malikisi 2)
f. Perekani mutu wa nkhaniyi
_____________________________________________________________________________ (Malikisi 2)

GAWO C: (Malikisi 10)

Yankhani mafunso onse awiri m’gawoli.

4. Werengani kankhanika ndipo muyankhe mafunso otsatirawo

Wotsogolera, “Mayendedwe athu ali motere. Abusa patsogolo ndipo ena tonse titenga mfumu yathu tikuyenda
pang’onopang’ono ulendo wopita kumudzi.

©CZ2023 Page 3 of 7
MAFUNSO

(i) Kodi ndi malonje anji mwawerengawa?


___________________________________________________________________ (Malikisi 1)
(ii) Kodi mawu oti kumudzi akutanthauza chiyani?
___________________________________________________________________ (Malikisi 1)
(iii) Kodi nyumba yochitikira mwambo ngati umenewu imatchedwa chiyani?
___________________________________________________________________ (Malikisi 1)
(iv) Munthu akavala zovala zakuda zokhazokha zimatanthauzanji?

___________________________________________________________________ (Malikisi 1)
(v) Lembani mwambi umodzi umene umanenedwa kawirikawiri pa mwambo ngati umenewu.

______________________________________________________________________(Malikisi 1)
5. KUPANGA ZIGANIZO
Pangani ziganizo zomveka bwino ndi mawu otsatirawa
(i) mothimbwizika
_________________________________________________________________________________
(ii) wonenepa
_________________________________________________________________________________
(iii) saka
_________________________________________________________________________________
(iv) futsa
_________________________________________________________________________________
(v) khwimbi
_________________________________________________________________________________

GAWO D (Malikisi 40)


Mafunso 6 mpaka 15: Sankhani mitundu ya D. Muonjezi
mawu amene atsekedwa mzere kunsi kwawo 8. Jonasi amakonda atsikana aafupi
mziganizo zotsatirazi. okhaokha.
6. Bauleni wadzimenya yekha. A. Mneni
A. Dzina B. Mlowammalo
B. Mfotokozi C. Muonjezi
C. Mlowammalo D. Mfotokozi
D. Muonjezi 9. Zoonadi ndatola ndine.
7. Mdengu muli Malalanje ambiri. A. Muonjezi
A. Mperekezi B. Mperekezi
B. Mlumikizi C. Mneni
C. Mneni D. Mlumikizi

©CZ2023 Page 4 of 7
10. Uthawe ndi ife. 17. Chikondi azidzakahala kuno.
A. Mneni A. Yakale yopitilira
B. Mperekeziu B. Yatsopano
C. Mlumikizi C. Yamtsogolo
D. Mvekero D. Yamtsogolo yopitilira
18. Ndidyabe ndikamva njala.
Mafunso 11 mpaka 15: Sankhani magulu a A. Yamtsogolo yathayi
mayina omwe atsekedwa nzere kunsi kwawo B. Yatsopano
mziganizo zotsatirazi. C. Yatsogolo
11. Cheke D. Yatsogolo yopitilira
A. Mu, - Mi 19. Tizidzavina naye usiku.
B. Mu, - A A. Yamtsogolo yopitilira
C. I, - Zi B. Yamtsogolo
D. Chi, - Zi C. Yamtsogolo yakawirikawiri
12. Mtungo D. Yatsopano yangothayi
A. Mu, - Mi 20. Tione adapita kumudzi.
B. Mu, - A A. Yakale yopitilira
C. Li, - Ma B. Yakale
D. I, - Zi C. Yakale yangothayi
13. Mphuno D. Yatsopano yangothayi
A. Mu, - Mi
B. Ka, - Ti Mafunso 21 mpaka 25: Sankhani mawu ofanana
C. Mu, - A mmatanthauzo ndi omwe atsekedwa nzere kunsi
D. I, - Zi kwawo mziganizo zotsatirazi.
14. Mudzi 21. Ife kwanthu tadya nsawa.
A. Mu, - A A. Nkhobwe
B. Li, - Ma B. Mtedza
C. Ku, - Pa, - Mu C. Nandolo
D. Mu, - Mi D. Mphalabungu
15. Kudya 22. Chaka chino ndilima mbwanda zambiri.
A. Ku, - Pa, - Mu A. Mbwani
B. Ku + tsinde la mneni B. Nyemba
C. I, - Zi C. Khobwe
D. U, - Ma D. Nandolo
23. Watenga chimungulu change ndani?
Mafunso 16 mpaka 20: Sankhani nthawi ya aneni A. Mbatata
omwe ali ndi mzere kunsi kwa ziganizo B. Chirazi
zotsatirazi. C. Nzama
D. Chinangwa
16. Iye wadya mbatata. 24. Pamudzi pa a Chuma panali chaka
A. Yakale yathayi chadzaoneni.
B. Yatsopano A. Mphwando
C. Ya mtsogolo B. Chisangalalo
D. Yatsopano yathayi C. Mpungwempungwe

©CZ2023 Page 5 of 7
D. Gule A. Mtengo
25. Iye wadya zingwa zitatu yekha. B. Ng’ombe
A. Mbatata C. Dothi
B. Chinangwa D. Madzi
C. Buledi 33. Ndiine owopsa koma madzi anditha
D. Mapapaya mphamvu.
A. Moto
Mafunso 26 mpaka 30: Sankhani mawu amene B. Nsima
akusutsana mmatanthauzo ndi omwe ali ndi nzere C. Dzuwa
kunsi kwawo mziganizo zotsatirazi. D. Dothi
26. Ife tadya kadzutsa. 34. Alendo m’mawa masana apita.
A. Mgonero A. Mvula
B. Nkhomaliro B. Misonzi
C. Mfinsulo C. Mame
D. Madyelero D. Madzi
27. Makedzana anthu ankavala nyanda. 35. Bwana waponda dona, dona wati “Yesi”
A. Nkucha A. Minga
B. Makono B. Masamba aawisi
C. M’bandakucha C. Mzungu
D. Kale D. Masamba owuma
28. Nasibeko waphika nyemba.
A. Waphula Mafunso 36 mpaka 40: Sankhani matanthauzo a
B. Wateleka zining’a mziganizo zotsatirazi.
C. Wagawa 36. Ndamuona tenthandizime uja akupita kwa
D. Wavundukula Nabanda.
29. Mbava zikagwidwa zimaona zodamutu. A. Woyendayenda
A. Mavuto B. Kazitape
B. Nzeru C. Wosamvera makolo
C. Tsoka D. Wachipongwe
D. Mwayi 37. Kondwani wapakidwa chipere.
30. Utchisi ndi wosafunika pasukulu. A. Wanamizidwa
A. Usiwa B. Wanyozedwa
B. Ulamuliro C. Wanenedwa ndi anzake
C. Ukhondo D. Wanamizilidwa kuba
D. Ulemu 38. Dula phazi.
A. Munthu wodanitsa
Mafunso 31 mpaka 35: Sankhani matanthauzo a B. Leka kupitako
ndagi/zilapi zotsatirazi C. Pusitsa
31. Agogo anga Malaya awo ndi minga. D. Pwetekana
A. Chisoni 39. Mlenje uyu ndi kanga ndiwamba.
B. Kamba A. Wosamvera
C. Nungu B. Kudyera zankhuli
D. Kalulu C. Munthu wonama
32. Kanditema bala siliwoneka. D. Wolongolola

©CZ2023 Page 6 of 7
40. Mnyamata uja adadya matako agalu. D. Tinkhunda
A. Munthu wonama 43. Nkhuku
B. Munthu woyendayenda A. Tambala
C. Munthu wokonda kudya nyama B. Msoti
D. Munthu womwa mowa C. Chipsolopsolo
D. Mwanapiye
Mafunso 41 mpaka 45: Sankhani zazing’ono za 44. Ndoda
mayina otsatirawa. A. Mphongo
41. Galu B. Akuluakulu
A. Mphonda C. Kamuna
B. Pope D. Zimphona
C. Mphongo 45. Ng’ombe
D. Kagalu A. Msona
42. Nkhunda B. Msoti
A. Mbalame C. Tonde
B. Unda D. Nkhunzi
C. Njiwa

MAFUNSO ATHERA APA

©CZ2023 Page 7 of 7
STD 7: MAYANKHO – CHICHEWA
1. Chimangirizo
kapena
2. Kalata
3. KUMVETSA NKHANI B
a. Atsibweni ake a Magireti
b. Kuphika zakudya komanso kuyimba nyimbo
c. A Patheretu
d. (i) Nyumba yokambirana
(ii) Perekeza
(iii) Kufunsana mafunso
e. (i) Mphika
(ii) Malovu

4. MALONJE
a. Apa maliro
b. Kumanda
c. Siwa
d. Chisoni kapena namfedwa
e. Kuziwa mnzako mkuziwa malo omwe iye wagona/amakhala
5. KUPANGA ZIGANIZO
 Ophunzira apange ziganizo zomveka bwino. Chiganizo chiyambe ndi lembo lalikulu ndipo chimalize ndi
mpumiro.

GAWO D

6. C 16. A 26. A 36. B


7. D 17. D 27. B 37. A
8. D 18. C 28. A 38. B
9. A 19. A 29. D 39. C
10. C 20. B 30. C 40. B
11. D 21. B 31. C 41. A
12. A 22. B 32. D 42. B
13. D 23. A 33. A 43. D
14. D 24. B 34. C 44. C
15. B 25. C 35. D 45. A

Page 8 of 8
STUDENT NAME ________________________________________________________________________ STD 5
MPHANDE ZONE EXAMINATIONS BOARD
2024 STANDARD FIVE END OF TERM TWO EXAMINATION
CHICHEWA
(100 MARKS)
SCHOOL NAME:_____________________________________________________

GAWO A (30 MARKS)


1 Lembani chimangirizo pa mutu oti “masewero omwe ndimawakonda” Mwa zina
tsatirani izi polemba chimangirizo chanu
Ndime yoyamba
 Tchulani dzina la masewero omwe mumawakonda
 Kodi masewerowo amseweredwa nthawi yanji
Ndime yachiwiri
 Kodi masewerawa amasewera anthu angati
 Tchulani malo omwe masewerowa amaseweredwa
Ndime yachitatu
 Fotokozani kufunika kwa masewero omwe mumawakondawo
 Tchulani chomwe chimakusangalatsani pamasewerowo

GAWO B (20 MALIKISI) KUMVETSA NKHANI


2 Werengani nkhani yotsatira mosamala kenako muyankhe mafunso otsatirawo
M’mudzi wina mudali abambo awiri mayina awo adali a Tenthenai ndi a Juma. Tsiku lina
usiku nyumba zawo zidaloshoka ndi mvula yamkutho. M’mawa kutacha, abambowa adaganiza
zokagula mitengo kumudzi kwa malango. Adatero chifukwa choti m’mudzi mwawo mitengo
idali itatheratu.
Iwowa atafika m’mudzi mwa a Malango adakumanizana ndi msonkhano wokhudza za
kusamalira zachilengedwe. Abambowa adamva za kuipa kodula mitengo ndi kutentha tchire ndi
momwe angasanalire mitengo monga kulambulira njira mozungulira nkhalango komanso
kubzala ina ndi kusatentha tchire.

Page 1 of 6
STUDENT NAME ________________________________________________________________________ STD 5
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________

Page 2 of 6
STUDENT NAME ________________________________________________________________________ STD 5
Mafunso
a. Tchulani mayina azibambo awiri omwe adakagula mitengo kwa amalango
________________________________________________________________________
_____________________________________________________________ (4 malikisi_
b. Perekani zifukwa ziwiri zomwe azibambowa adakagulira mitengo kwa malango
________________________________________________________________________
_____________________________________________________________ (4 malikisi)
c. Fotokozani njira ziwiri zosamalira mitengo
________________________________________________________________________
____________________________________________________________ (4 malikisi)
d. Perekani mawu ofanana matanthauzo ndi awa .
i. Mvula yamkutho ________________________________________ (2 malikisi)
ii. Loshoka _______________________________________________ (2 malikisi)
e. Lembani mutu wa nkhaniyi
____________________________________________________________ (4 malikisi)

GAWO C ( MALIKISI 20)


3 werengani kankhanika ndipo muyankhe mafunso otsatirawa.

Gwaza: Ena alowe. Ndikuthandizeni bwanji bambo


Zagwa: Thupi likungophwanya komanso ndikumamva kuzizira kwambiri.
Gwaza: Gonani apo ndikupimeni

a. ndi malonje anji alikankhanika


_________________________________________________________ (2 malikisi)

b. kodi a Gwaza ndi ndani mumalonjewa?


_________________________________________________________ (2 malikisi)

c. Perekani mawu ofanana matanthauzo ndi kupima


_________________________________________________________ (2 malikisi)

Page 3 of 6
STUDENT NAME ________________________________________________________________________ STD 5
d. Tchulani malo omwe anthuwa akuyankhulirana
_________________________________________________________ (2 malikisi)

e. Kodi kuvula chipewa podutsana ndi akulu kumatanthauza chani


________________________________________________________ (2 malikisi)

4 KUPANGA ZIGANIZO
Pangani ziganizo zomveka bwino ndi mawu kusonyeza kuti mukudziwa matanthauzo ake
i. Loshoka
______________________________________________________________________
ii. Kuzambwe
______________________________________________________________________
iii. Pamgong’o
______________________________________________________________________
iv. Ziphe
______________________________________________________________________
v. Vina
______________________________________________________________________

(10 malikisi)
GAWO D (MALIKISI 40 )
Mafunso 5 mpaka 9 sankhani mawu oyenera 7 Kuwala ngati ___________
kutanthauza zifanifani zotsatirazi A. Dzuwa
B. Nyali
5 ___________ ngati chitedze
C. Nkhope
A. There’re
D. Pepala
B. Kuyera
C. Kuyabwa
8 _______ kutalika ngati akalulu
D. Mkango
A. Mwendo
6 Kuyipa mawu ngati __________
B. Tsitsi
A. Chule
C. Mvula
B. Fisi
D. Makutu
C. Kalulu
D. Galu
Page 4 of 6
STUDENT NAME ________________________________________________________________________ STD 5
9 Kukonda mmadzi ngati _____ 14
A. Nsomba A. Ogo ufa uja watayika.
B. Ng’ona B. Ogo! Ufa uja watayika.
C. Chule C. ogo! Ufa uja watayika
D. Bakha D. ogo ufa uja watayika?
Mafunso 10 mpaka 14 sankhani chiganizo Mafunso 15 mpaka 19 sankhani mitundu ya
chomwe chili ndi zizindikiro zoyenera mawu oomwe atsekedwa mzere kunsi
kwawo
10
A. juliyasi wadya nsima. 15 Mwana walephera mayeso
B. Juliyasi wadya msima. A. Dzina
C. juliyasi wadya nsima B. Mfotokozi
D. Juliyasi wadya nsima. C. Muonjezi
D. Lokhudzika
11
A. joni wapiti kuti. 16 Nthaka yoguga sibeleketsa
B. Joni wapiti kuti A. Mlowawamalo
C. Joni wapiti kuti? B. Mfotokozi
D. joni wapiti kuti? C. Muonjezi
D. Mneni
12
A. Ine ndimadya mtedza, nthochi, 17 Iye wabwera dzulo
mbatata ndi mango A. Dzina
B. ine ndimadya mtedza, nthochi B. Mfotokozi
mbatata ndimango C. Mlowammalo
C. ine ndimadya mtedza nthochi, D. Mneni
mbatata ndi mango.
D. ine ndimadya mtedza, nthochi, 18 Amayi apita kumunda
mbatata ndi mango A. Mlowamalo
B. Mfotokozi
13 C. Dzina
A. mmadzimu mwagwera D. Mneni
mphemvu
B. mmadzimu mwagwera 19 Chifundo ndi Chisomo apita kusukulu
Mphemu. A. Mlumikizi
C. Mmdzimu mwagwera B. Muonjezi
Mphemvu C. Mfotokozi
D. M’madzimu mwa gwera D. Mlowamalo
mphemvu.

Page 5 of 6
STUDENT NAME ________________________________________________________________________ STD 5
Mafunso 20 mpaka 24 sankhani mayankho a
zilapi zotsatirazi 22 Walira wopanda matutumbo
A. N’goma
20 Agogo anga aimvi m’mimba
B. Chiwala
A. Udzu
C. Mtengo
B. Malambe
D. Dzira
C. Lamba
D. Mphonda
23 Kamwana kakang’ono kaimitsa
amfumu
21 Diwa lansenjere kugwaigwa
A. Moto
A. Nkhwangwa
B. Tsabola
B. Nsima
C. Minga
C. Chikope
D. Chisoso
D. Mano
24 Sudzi, nkuphompho
A. Madzi
B. Mvula
C. Lilime
D. Mamina

MAFUNSO ATHERA APA

Page 6 of 6
EXAMINATION NO.:____________________________

CHAMBE ZONE EXAMINATION BOARD


2022 STANDARD MOCK EXAMINATION
CHICHEWA
100 MARKS
Subject Number:
Tuesday, 1st March, 2022 Time allowed: 2hrs 15mins
(8am – 10:15am)

Dzina lanu:________________________________________________________________________

Dzina la sukulu yanu:________________________________________________________________

Malangizo:
 Onetsetsani kuti kuti pepala ili lili ndi Question Tick if Do not write
masamba asanu ndi atatu. number answered anything in
 Lembani dzina lanu ndi la sukulu yanu pa these columns
mipata ili mwambayi.
1
 Lembani nambala yanu ya mayeso pa mpata
2
omwe uli pa pamwamba pa tsamba lililonse.
3
 Pepala ili lili ndi magawo anayi A, B, C ndi
4
D.
5
 Lembani kalata kapena chimangirizo mu
6
gawo A ndipo yankhani mafunso onse mu
6 - 10
gawo B, C ndi D.
11 – 15
 Chongani mu bokosi lomwe lili ku
16 – 20
kutsogolo kwa mafunso omwe mwayankha.
20 - 25
 Pelekani pepala lanu kwa oyang’anira
mayeso (invigilator) nthawi yolembera
mayeso ikatha.

© 2022 CHAZEB Turn over/…..

1
EXAMINATION NO.:____________________________

GAWO A: (Malikisi 30)

Langizo: Yankhani funso limodzi lokha mwa mafunso ali m’musiwa. Sankhani mutu wa
chimangirizo kapena wa kalata. Mawu a chimangirizo chanu kapena kalata asachepere
100 koma asabzole 150.
1. Lembani chimangirizo pa mutu uwu “GULE WA KWATHU”
Ndime yoyamba
 Dzina la gule yemwe amavinidwa kwanu
 Anthu omwe amavina guleyu
 Nyengo imene guleyu amavinidwa
Ndime yachiwiri
 Zovala zomwe zimavalidwa povina guleyu
 Zifukwa zovinira guleyu
 Ubwino wa guleyu
Ndime yachitatu
 Momwe mukulimbikitsira guleyu
KAPENA
2. Mwachotsedwa sukulu muli fomu 1 pa Litonga Sekondale Sukulu chifukwa cha
makhalidwe anu oipa. Lembani kalata kwa mphunzitsi wamkulu. Litonya
Sekondale Sukulu P.O. Bokosi 211 Zomba Yomupempha kuti mubwelerenso.Tsatani izi
polemba kalata;

Ndimbe yoyamba
 Tchulani tsiku ndi nthawi yomwe adakuchotsani sukulu
 Fotokozani zifukwa zomwe adakuchotserani
Ndime yachiwiri
 Zovuta zomwe mukukumana nazo chifukwa chokuchotsani sukulu
 Zovuta zatsokoneza bwanji tsogolo lanu?
Ndime yachitatu
 Fotokozani momwe muzikhalira kusonyeza kuti mwasintha mukabwereranso
kusukulu.

____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________

2
EXAMINATION NO.:____________________________

____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
____________________________________________________________________________________
3
EXAMINATION NO.:____________________________

GAWO B: (Malikisi 20)

KUMVETSA NKHANI
3. Werengani nkhani yotsatirayi mosamala kenako yankhani mafunso otsatirawa.

M’mudzi mwa Mbalame mudali nyamata dzina lake Kadyereni.Nyamatayi adali wamtali
dzala. Khalidweli adayamba oahkomo la amayi ake a Nadimba ndi a Chigwe. Ngakhale
makolo ake amamulangiza kuti khalidweli ndi loipa, Kadyereni zonsezi amazitayira
kunkhongo. Atalemba mayeso ake a sitandade 8, Kadyereni adapita ku sukulu yogonera
komweko komwe adapitiliza umbava wake pobera anzake mabuku, sopo komanso
ndalama.

Poti chozemba chidakumana ndi chokwawa, tsiku lina Kadyereni adagwidwa akuba
ndipo ophinzira anzake adakamuneneza kwa mphunzitsi wamkuluyemwe adampatsa
chilango cholapitsa kuti asinthe chikhalidwe chake koma iye sadasinthe.

Aphunzitsi adathedwa naye nzeru ndipo adamuchotsa sukulu. Ali kumudzi kwawo
Kadyereni sadasiyebe umbava. Iye amaba mnyumba za anthu komanso m’sitolo za
mm’udzimo. Tsiku lina adagwidwa apa ndiye anaona zakuda ndipo adakumbukira
malangizo omwe makolo adampatsa, poti mawu aakulu akoma akagonera. Apolisi
atamva za Kadyereni sadazengereze koma kupita kukamunjata. Mbiri ya kugwidwa
komanso kumenyedwa kwa Kadyereni ikudamveka ponseponse ndipo adatsekeredwa
m’chitolokosi cha apolisi. Ana onse adadziwa kuti umbava ndi oipa umayikitsa moyo
pachiswe.

Tsopano yankhani maunso otsatirawa.

a. Kodi kwawo kwa Kadyereni kudali kuti?


______________________________________________________________________(1malikisi)
b. Kodi Kadyereni umbava adayambira kuti?
_____________________________________________________________________ (1malikisi)
c. Tchulani zinthu ziwiri zomwe Kadyereni amawabera anzake kusukulu.
_____________________________________________________________________ (2malikisi)
d. Pezani mkuluwiko ofanana m’matanthauzo ndi uwu “onyalanyaza”
______________________________________________________________________ (1malikisi)
e. Fotokozani zomwe mphunzitsi wamkulu adamuchitira Kadyereni.
_________________________________________________________________________________
______________________________________________________________________ (2malikisi)
f. N’chifukwa chiyani Kadyereni adamuonetsa zakuda?
_________________________________________________________________________________
______________________________________________________________________ (2malikisi)
g. Mukuganiza kuti chifukwa chiyani a polisi sadachedwe kukamunjata Kadyereni?
_________________________________________________________________________________
______________________________________________________________________(2malikisi)
h. Pezani matanthauzo a mikuluwiko iyi:
i) kuthedwa nzeru
_____________________________________________________________________ (1malikisi)
4
EXAMINATION NO.:____________________________

ii) chozemba chinakumana ndi chokwawa


_____________________________________________________________________ (1malikisi)
i. Perekani phunziro lomwe mwapeza m’nkhaniyi
_________________________________________________________________________________
______________________________________________________________________ (1malikisi)
j. Perekani mawu osutsana m’matanthauzo ndi awa:
i) kumbukira ________________________________________________________ (1malikisi)
ii) mangidwa________________________________________________________ (1malikisi)
k. Perekani mutu wa nkhaniyi
_____________________________________________________________________ (2malikisi)

GAWO C: (Malikisi 10)


4a. Werengani kankhanika ndipo muyankhe mafunso otsatirawoa

“Chaka chino ndaganiza mozama. Ndikufuna kuti tonse tibzale mbewu ya makono
yachimanga kuti m’mudzi muno musadzadutsenso galu wakuda.”

Mafunso

i) Ndi malonje anji amenewa?


_____________________________________________________________________ (1malikisi)

ii) Kodi malonjewa akuyankhulidwa kwa yani?


______________________________________________________________________(1malikisi)
iii) Mawu oti “galu wakuda” akutanthauzanji?
______________________________________________________________________ (1malikisi)
b. Kodi pamsewu nyali yachikasu imatanthauzanji?
______________________________________________________________________ (1malikisi)
c. Perekani njira imodzi yotumizira uthenga wa ukwati.
______________________________________________________________________ (1malikisi)

5. Kupanga ziganizo.
Pangani ziganizo zomveka bwino ndi mawu awa:
a. tchona
______________________________________________________________________ (1malikisi)
b. thimbwizika
______________________________________________________________________ (1malikisi)
c. mbee
_______________________________________________________________________(1malikisi)
d. mbutuma
______________________________________________________________________(1malikisi)
e. chitete
______________________________________________________________________(1malikisi)

5
EXAMINATION NO.:____________________________

GAWO D
Zungulitsani lembo lokhonza (A,B, C Kapena D) m’mafunso otsatirawa.

Mafunso 6 mpaka 10: Sankhani B. yatsopano yopitilira


mitundu a mawu omwe atsekedwa mzere C. yamtsogolo yathayi
kunsi kwawo. D. yatsopano yathayi yopitilira.
6. Mkango ndi chilombo choopsa.
A. Mlumikizi C. Mperekezi 15. Iwo amalima mpunga.
B. Mvekero D. Mneni A. Yatsopano akawirikawiri
B. yamtsogolo
7. Moyo umenewu siwabwino. C. yakale
A. Dzina C. Mvekero D. yatsopano yathayi yopilira
B. Mneni D. Mfuwu
8. Imodzi apezeka m’nyumba ya a Mafunso 16 mpaka 18: Sankhani mawu
Bwande. otsutsana m’matanthauzo ndi omwe
A. Mfotokozi C. Dzina atsekedwa mzere kunsi kwawo.
B. Mlowam’malo D. Muonjezi
16. Banja ilo lili pa chisoni.
9. Amayi amandikaniza kupita kutali. A. Pa chikondi C. Pa mtendere
A. Mfotokozi C. Mperekezi B. Pa ufulu D. Pa chimwemwe
B. Dzina D. Muonjezi
10. Achule amakhala m’madzi 17. Ife ndife nzika za M’malawi.
A. Dzina C. Muonjezi A. mfulu C. mlendo
B. Mperekezi D.Mlumikizi B.kapolo D. mkamwini

Mafunso 11 mpaka 15: Sankhani 18. Umphawi wafika povuta kwambiri.


mutundu ya nthawi za aneni yomwe A. Utchisi C. Ukapolo
yatsekedwa mzere kunsi kwawo. B. Ulemelero D. Umbanda

11. Amisiri akumanga nyumba. 19. Iwo mapita ku sukulu kuti


A. yatsopano yathayi akaphunzire kulemba.
B. yatsopano A. yoima payokha
C. yatsopano yopitilira B. yadzina
D. yatsopano yakawirikawiri C. yamfotokozi
D. yamuonjezi
12. Belita anali ataweruka pamene
amchita ndewu 20. Ng’ombe yomwe waphayi ndi
A. yatsopano yopitilira yanga.
B. yakale opitilira A. yadzina D. yoyima payokha
C. yakale yathayi B. yamfotokozi C. yadzina
D. yatsopano yathayi
21. Zomwe mwapatsidwazo ndi
13. Chimango abagulitsa chinangwa. zofunika kwambiri.
A. yatsopano A. yadzina C. yamuonjezi
B. yamtsogolo B. yamfotokozi D. yoima payokha
C. yakale
D. yamtsogolo yopilira
Mafunso 22 mpaka 26: Sankhani
matanthauzo a mikuluwiko
14. Atsikana akuvina chioda.
A. yamtsogolo yopitilira yotsatirayi.

6
EXAMINATION NO.:____________________________

Mafunso 27 mpaka 30: Sankhani


22. Suzumire adaphetsa mkhalakale. magulu a mayina omwe ali ndi
A. Sibwino kuchita zinthu mzere kunsi kwawo.
mwachangu
B. Anthu okalamba amafa 27. Wanyamula katoni ya sopo.
mwadzidzidzi. A. Mu-, Mi- C. Li-, Ma-
C. Kusaugwira mtima kumadzetsa B. Ka-, ti- D. Mu-, A-
mavuto.
D. Kusasamala kumaonongetsa 28. Ng’ombe zathawira m’tchire.
zinthu. A. Ku-, Pa-, Mu-
B. Ku- ndi tsinde la Mneni
23. Chifundo chidaphetsa Msema C. Mu-, Mi-
mitondo. D. Chi-, zi-
A. Sibwino kukhala ndi luso
lapadera 29. Atate amadana ndi mwambo wa
B. Chifundo chimaiwalika pa chinamwali.
mavuto A. I-, Zi- C. Mu-, Mi-,
C. Ntchito iliyonse ili ndi mavuto B. Li-, Ma- D. U-, Ma-
ake.
D. Chifundo nthawi zina 30. Mafuli adandibera uchi wanga.
chimapweteketsa. A. Chi-, Zi- C. Mu-, Mi-
B. Mu-, A- D. U-, Ma-
24. Nkhondo ndi anansi.
A. Abale amatikonda pamtendee Mafunso 31 mpaka 35: Sankhani
pokha. chiganizo chomwe chili ndi zizindikiro za
B. Abale nthawi zina amafunirana m’kalembedwe zoyenera.
zoipa.
C. Abale nthawi zina sayamika. 31. A. Kodi mnkhaniyi
D. Abale saoneka pa mavuto. mwaphunziramo chiyani?
B. Kodi m’nkhaniyi
25. Taya udzu omwetamweta. mwaphunziramo chiyani?
A. Kusachitapo kanthu mavuto C. Kodi mn’khaniyi
ukawaona. mwaphunziramo chiyani?
B. Kusadziwa chochita pa mavuto. D. Kodi m’nkhaniyi
C. Kusagwiritsa ntchito mwayi mwaphunziramo, chiyani?
opezapeza.
D.Kusazindikira kuti uli ndi nzeru 32. A. Mnyamata iwe penyetsetsa kuti
za padera. uwone zenizeni.
B. Mnyamata iwe! Penyetsetsa kuti
26. Ndionetsetse adathetsa nkhosa. uwone zenizeni.
A. Kuzengereza kumapezetsa C. Mnyamata iwe, Penyetsetsa kuti
mavuto. uwone zenizeni.
B. Changu chimapezetsa mavuto. D. Mnyamata iwe. Penyetsetsa kuti
C. Ukaona zinthu uziuza anzako. uwone zenizeni.
D. Tizionetseta zinthu
tisanachitepo kanthu.

7
EXAMINATION NO.:____________________________

33. A. Ndi liti? Duwa lomwe C. Wochitirana


silinapsonthedwe. D. Onyazitsa
B. Ndi liti duwa lomwe
silinapsonthedwe? 39. Penyetsetsa kuti uwone zenizeni.
C. Ndi liti! Duwa lomwe? A. Wochititsa C. Wochititsitsa
silinapsonthedwe B. Wochitidwa D. Owonetsetsa
D. Ndi liti duwa lomwe
silinapsonthedwe!
40. Atsikanawo amenyerana
34. A. Mbale zili mbwe! pabwalo. mwamuna.
B. Mbale zili mbwe, pabwalo. A. Wochititsa
C. Mbale zili mbwe pabwalo. B. Wochitidwa
D. Mbale, zili mbwe pabwalo. C. Wobwerezabwera
D. Wochitirana
35. A. Chifukwa cha njala iye adamwa
zakumwa zone. Mafunso 41 mpaka 45: Sankhani
B. Chifukwa cha njala iye, adamwa matanthauzo oyenera a zilapi izi.
zakumwa zone.
C. Chifukwa cha njala iye adamwa, 41. Mfuti yanga yoalsira kumbuyo
zakumwa zone. A. tombolombo C. ntchentche
D. Chifukwa cha njala, iye B. njuchi D. nthonga
adamwa zakumwa zone.
42. Mbalame yoikira paminga.
Mafunso 36 mpaka 40: Sankhani A. mutu C. lilime
msintho wa aneni omwe atsekedwa B. mano D. maso
mzere kunsi kwa ziganizo zotsatirazi.
43. Muvi wa atate chiboola tsindwi
36. Anawa adaleledwa bwino. A. utsi C. lilime
A. Wochitidwa C. Wochitirana B. mpaliro D. mano
B. Wochititsa D.Wochititsitsa
44. Nyama pamwamba, chikumba
37. Osewera onse amavala Malaya mkati.
ofanana. A. chiwindi C. chikhadabo.
A. Wochititsa C.Wobwerezabwereza B. chivututu D. mango
B. Otsutsa D. Wochitidwa
45. Amayi tsalani kunyumba ndipita
38. Anthu ena amatolatola zinthu za ndi ine.
eni. A. chimanga C. mapesi
A. Wobwerezabweraza B. masamba D. mwana
B. Wochitira

MAFUNSO ATHERA PANO

8
STUDENT NAME __________________________________________________________________ STD 7
MPHANDE ZONE EXAMINATIONS BOARD
2024 STANDARD SEVEN END OF TERM TWO EXAMINATION
CHICHEWA
(100 MARKS)
SCHOOL NAME:_____________________________________________________

GAWO A (30 MARKS)


Yankha funso limodzi lokha mwa mafunso awiri ali m’musiwa, sankhani mutu wa
chimangirizo kapena wa kalata.
1. Lembani chimangirizo pa mutu uwu “Ntchito yomwe ndikufuna ndidzagwire” Mwa
zina tsatani izi polemba
Ndime yoyamba
 Ntchito yanji yomwe mukufuna mudzagwile mukadzamaliza sukulu?
 Nchifukwa chiyani mukufuna mudzagwire ntchito imeneyi?
Ndime yachiwiri
 Ndindani yemwe akugwira ntchito ngati yomweyi m’dera lanu?
 Ndizosangala ziti zomwe iye adachita zomwe zidapangitsa kuti muyambe kuganiza za
ntchitoyi.
Ndime yachitatu
 Zofunika kuchita padakali pano kuti mudzapeze ntchito n’chiyani?
 Kodi ndichilimbikitsa chotani chomwe mukulandira kuchokera kwa makolo komanso
achibale?
KAPENA
2. Lembani kalata kwa nzanu yemwe akukhala kunja kwa dziko lino yomufotokozera za
chitukuko chomwe chikuchitika mdera lanu.
Ndime yoyamba
 Kukuchitika chitukuko chanji?
 Chikuchitikira mmudzi wanji?
Ndime yachiwiri
 Adabweretsa chitukukochi ndi ndani?
 Nchifukwa ninji adaganiza zokhazikitsa chitukukochi?
 Padakali pano zikuchitika nzotani zokhuzana ndi chitukukochi
Ndime yachitatu
 Chikatha kukozedwa chitukukochi chizathandiza deralanu motani.
Page 1 of 8
STUDENT NAME __________________________________________________________________ STD 7
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
_____________________________________________________________________________
Page 2 of 8
STUDENT NAME __________________________________________________________________ STD 7
GAWO B (MALIKISI 20 ) KUMVETSA NKHANI
3. Werenkhani nkhani yotsatirayi mosamala kenako muyankhemafuinso otsatirawo
M’mudzi mwa a chimulango mudali mtsikana wotchedwa madalo. Atate ake a madalo, Mlera
adamwalira iye adakali m’chikuta. Mwanayi adareledwa ndi mchimwene wake yemwe amgwira
ntchito ku kampani ya zomangamanga kutawuni. Madalo adali mwana womvera ndi waulemu.
Kusukulu kwake adali kuchita bwino m’maphunziro ake.
Tsiku lina atsibweni a madalo adabwera kuchokekutawuni. “Chemwali ine kubweraku
ndikufuna kuti Madalo ndimutenge ndipite naye kutawuni Ntchito zapakhomo zikundisautsa
kwambiri. Ndikufuna kuti madalo asiye sukulu azikandiphikira, kuchapa zovala ndikugwira
ntchito zina zapakhomo. Ndikhulupilira kuti adagwa kale dothi ndipo akakachita mwayi
ndikamukwatiritsa kutawuni komweko. Nanga inu chemwali mukuti chiyani pankhaniyi?
Mayankho ali ndi mwini wake Madalo. Atamufunsa Madalo adati Atsibweni ine ndamva zonse
zomwe mwanena koma mundipatse mpata kuti ndiganize mofatsa. Ndidzakulemberani kalata
posachedwa. Mkalatamo ndidzafotokoza maganizo anga pankhaniyi.
Usiku wa tsiku limenero Madalo sadagone tulo tokwanira iye sadagwirizane ndi zomwe
adanena atsibweni ake aja. M’mawa kutacha adalemba kalata kwa atsibweni ake
yowafotokozera zokana kupita kutawuni cholinga amalize kaye sukulu.
MAFUNSO
a. Tchulani dzina la atate a Madalo?
______________________________________________________________(2 malikisi)
b. Kodi achimwene a Madalo amagwira ntchito yanji?
______________________________________________________________ (2 malikisi)
c. Tchulani mudzi womwe amakhala Madalo
______________________________________________________________ (2 malikisi)
d. N’chifukwa chiyani atsibweni a Madalo adapita kumudzi?
______________________________________________________________ (2 malikisi)
e. Kodi madalo adawayankha zotani atsibweni ake?
______________________________________________________________ (2 malikisi)
f. Kodi atsibweni a Madalo amakhala kuti?
______________________________________________________________ (2 malikisi)
g. Perekani manthauzo a mawu awa
i. M’chikuta ________________________________________________________
ii. Kugwa dothi ______________________________________________________
h. Perekani mawu ofanana matanthauzo ndi atsibweni
______________________________________________________________ (2 malikisi)
i. Lembani mutu wankhaniyi
______________________________________________________________ (2 malikisi)
Page 3 of 8
STUDENT NAME __________________________________________________________________ STD 7
GAWO C (20 MALIKISI)
4. Werengani kakhani kotsatiraka posiliza muyenkhe mafunso.

Angozo : Odi! Odi! Phiri


Phiri : EEh! Tiwaope?
Angozo : Ayi asatiope kwenikweni.
Kungoti kumudzi kwathu
Kuli katambala. Ndiye kakuti kadaona kansoti pa mudzi panopa.
Mafunso
1 Ndi malonje anji ali nkankhanika?
________________________________________________________________
2 Kodi Angozo ndi ndani
________________________________________________________________
3 Malonjewa akuchitikira kuti?
________________________________________________________________
4 Malonjewa akuchitikira kuti?
________________________________________________________________
5 Nchifukwa chiyani asungwana ayenera kugwada poyankhula ndi akuluakulu?
________________________________________________________________
6 Tchulani malo amodzi komwe tingapeze madzi.
________________________________________________________________

Kupanga ziganizo
5. Lembani ziganizo zomveka bwino ndi mawu otsatirawa

a. Bungwe
________________________________________________________________
b. Zonda
________________________________________________________________
c. Tumbwa
________________________________________________________________
d. Yendetsa
________________________________________________________________
e. Lakalaka
________________________________________________________________

Page 4 of 8
STUDENT NAME __________________________________________________________________ STD 7
GAWO D (MALIKISI 40)
Mafunso 6 mpaka 10 sankhani mitundu ya 12. Amayi agula tambala
mawu omwe atsekedwa mzere A. Chipsolopsolo
B. Msoti
6. Mtsikanayo ndi wanzeru koma
C. Mkota
ndiwamwano
D. Thadzi
A. Mlumikizi
B. Mneni
13. Abwana anga athyoka mkono
C. Dzina
A. Anduna
D. Muonjezi
B. Mfumakazi
C. Mtengwa
7. Iye ndi mnyamata
D. Adona
A. Mneni
B. Mlowammalo
14. Tasauka chisodzera wakwathu
C. Mfotokozi
A. Buthu
D. Muonjezi
B. Mnyamata
C. Mtsikana
8. Tangatanga si nthenda
D. Mwana
A. Mneni
B. Muonjezi
15. Ameneyu akumane ndi atsibweni ake
C. Mvekero
A. Malume
D. Mlumikizi
B. Ndoda
9. Munthu uja akudwala
C. AZakhali
A. Muonjezi
D. Mwana
B. Mperekezi
C. Mneni Mafunso 16 mpaka 20 sankhani mawu
D. Mfotokozi ofanana matanthauzo ndi omwe atsekedwa
10. Maphunziro ndi ofunika kwambiri mzere
A. Dzina
16. Ana ambiri akumachita mtudzu
B. Muonjezi
A. Ulesi
C. Mlowammalo
B. Matama
D. Mneni
C. Mwano
Mafunso 11 mpaka 15. Sankhani chahikazi D. Dyera
cha zomwe zatsekedwa mzere.
17. Agogo aja apita ku masano
11. Mphulu ndi nyama yofatsa
A. Manda
A. Tonde
B. Kutchire
B. Msoti
C. Kuthengo
C. Nkhosa
D. Nkhalango
D. Thadzi
Page 5 of 8
STUDENT NAME __________________________________________________________________ STD 7
18. Angoni aberedwa mbwani m’munda 24. Kalulu wabisala ku una
A. Mpama A. U -, ma
B. Chinangwa B. Mu -, mi
C. Chilazi C. I -, zi
D. Mbatata D. Li -, ma

19. Ine ndadyera mbwanda zoyera 25. Iwo apezeka munda wa chinangwa
A. Nandolo A. Chi – zi
B. Buluwe B. Li – ma
C. Chipere C. I – zi
D. Nyemba D. Ka – ti

20. Dera lakwathu kuli dondo lalikulu.


Mafunso 25 mpaka 28 sankhani mawu
A. Chinangwa
ofanana m’matanthauzo ndi mawu omwe
B. Nkhalango
atsekedwa mzere kunsi kwawo mziganizo
C. Mtudzu
zotsatirazi.
D. Manda
26. Alimi ali pachionetsero cha zaulimi
A. Asodzi
Mafunso 21 mpaka 25 sankhani magulu a
B. Achikumbe
mayina omwe atsekedwa mzere
C. Alansizi
21. Panyanja pabuka namondwe D. Anganyu
A. Ka-,ti
B. I - ,zi 27. Malume aja abwera tsopano
C. Ku -, pa-, mu A. Agogo
D. Mu -, a B. Bamboo
C. Mumphwa
22. Boma la mwanza ndilokongola D. Atsibweni
A. Ka - ti
B. Mu -, a 28. Kumanda kukawirira kumachititsa
C. Li -, ma mantha
D. Chi - Zi A. Kunkhalango
B. Kugona
23. Kusamalira mitengo ndikwabwino C. Kutchire
A. U – ma D. Kuphanga
B. Mu – mi
C. Mu – a
D. I – zi

Page 6 of 8
STUDENT NAME __________________________________________________________________ STD 7
29. Kusintha mawanga ngati
birimankhwe 35. Amene wadya adwala
A. Tonkhwetonkhwe A. Waumwini
B. Nkhwadzi B. Wofunsa
C. Kamtema C. Wamgwirizano
D. Khwangwala D. Woloza
Mafunso 36 mpaka 40 sankhani mitundu ya
30. Kabawi wagwira mwanapiye
nthawi za aneni omwe atsekedwa mzere
A. Katawa
B. Nkhwadzi 36. Iye adali pano
C. Kamtema A. Nthawi yakale yamwinimwini
D. Khwangwala B. Nthawi yakale
C. Nthawi yatsopano
D. Nthawi yatsogolo
Mafunso 31 mpaka 35. Sankhani mitundu ya
alowam’malo omwe atsekedwa mzere kunsi
37. Mukaphunzira mudzidzasangalala
kwawo mziganizo zotsatirazi.
A. Nthawi yamtsogolo
31. Ine ndipita mawa B. Nthawi yamtsogolo yopitilira
A. Wotsimikiza C. Nthawi yopitiliza
B. Woloza D. Nthawi yatsopano
C. Waumwini
D. Wofula 38. Mwanayu amakonda kuyendaye
A. Nthawi yatsopano
32. Iwe sumva kamodzi B. Nthawi yatsogolo yathayi
A. Waumwini C. Nthawi yakale
B. Woloza D. Nthawi ya tsopano yopitilira
C. Wotsimikiza
D. Wopatula 39. Pepani ndachedwa ndimasamba
A. Nthawi yakale
33. ukufuna zotani? B. Nthawi yakale yanthayi
A. Woloza C. Nthawi yakale yopitiliza
B. Waumwini D. Nthawi yatsopano
C. Wamgwirizano
D. Wofunsa 40. Anawa ankadwala malungo
A. Nthawi yakale yathawi
34. Anayi agwera mmadzi B. Nthawi yakale
A. Wopatula C. Ntahwi yakale yathayi
B. Wowerenga yopitilira
C. Wamgwirizano D. Nthawi yakale yopitilira
D. Woloza
Page 7 of 8
STUDENT NAME __________________________________________________________________ STD 7
Mafunso 41 mpaka 45 tsilizani mikuluwiko
yotsatirayi
41. Ulenje umasimba __________ 43. Safunsa anadya __________
A. Wathu A. Phula
B. Wawo B. Mphutsi
C. Wako C. Mphaka
D. Waumwini D. Mkute

42. Khoswe akakhala pa _________ 44. Kandimverere adakanena ______


A. Mtsuko sapheka A. Mabodza
B. Nkhate sapheka B. Zoona
C. Moto sapheka C. Zenizeni
D. Mutu sapheka D. Zam’maluwa

45. Mapanga awiri


A. Amapasa
B. Amapha
C. Avumbwitsa
D. Anyowetsa

MAFUNSO ANTHERA APA

Page 8 of 8
NKHAMENYA ZONE EXAMINATION BOARD
2024 END OF TERM II EXAMINATIONS
STANDARD 7
CHICHEWA
(100 MARKS)
Name of Candidate:

Name of School: Time Allowed : 1hr and 30 mins

Malangizo

 Pepalali lili ndi magawo anayi (A, B, C ndi D) yankhani mafunso onse m’magawo onse.
 Lembani dzina lanu ndi nambala yanu pa malo omwe mwapatsidwa.

GAWO A (MALIKISI 30)

Langizo: lembani funso limodzi lokha mwa mafunso awiri a m’gawoli. Sankhani mutu
wachimangirizo kapena kalata.

Mawu achimangirizo kapena kalata yani asabzole 150 komanso asachepere 100.

1. Lembani chimangirizo pa mutu uwu: “usiku matenda omwe abuka m’dera lanu.
woopsa” Tsatirani izi polemba.

Ndime yoyamba Ndime yoyamba


 Udali usiku uti omwe mudawona  Cholinga cha kalata
zoopsa?  Ndinu ndani m’mudzimo?
 Zidachitika nthawi yanji?  Mtundu wa matendawo.
 Pa nthawiyi mumachita chiyani?
Ndime ya chiwiri
 Nanga mudali ndi yani?
 Nthawi yomwe matendawo
Ndime yachiwiri
adazindikilidwa
 Fotokozani zoopsa zomwe  Mudawona zizindikiro zanji?
zidachitikazo  Ndi anthu angati omwe
 Inu ndi anthu ena mudachita adakhudzidwa ndi matendawo?
chiyani?
Ndime ya chitatu.
Ndime ya chitatu
 Mudachita po chiyani pa zizindikiro
 Zidatha bwanji usiku umenewu? za matendawo?
 Zotsatira zake zidali zotani?  Mukufuna thandizo lanji kuchokera
kwa dotoloyo?
KAPENA  N’chifukwa chiyani mukufuna
2. Lembani kalata kwa dotolo pachipatala cha thandizolo?
Bilila, Bokosi 23, Bilila. Yomudziwitsa za
GAWO B (20 MALIKISI)
3. Werengani nkhani yotsatirayi kenaka yankhani mafunso otsatirawo.

Kalekale m’mudzi wa s Holla mudali nkhalango yaikulu yotchedwa Maliwati. Nkhalangoyi idali yowirira
kwambiri. Ponena mwatchutchutchu, nkhalangoyi idali yoopsa popeza mudali akambuku ndi mikango
komanso nkhalango yomweyi mudali nyama zina monga; akalulu, agwape, mphoyo ndi mphalapala.
Pafupi ndi nkhalangoyi padali mudzi wina dzina lake Zimema. M’mudzi muja mudali munthu wina dzina
lake Pingeni ndipo mkazi wake adali Naphiri. Pingeni adali katswiri pakupha nyama kuliwamba. Iye
amakonda kusaka yekha mu nkhalango muja. Ngakhale Naphiri amamulangiza kuti asamapite yekha
kokasaka, Pingeni samamvera.

Tsiku lilonse kukacha, Pingeni amapita kuliwamba ndi agalu ake. Iyeyu amapita kokasaka m’mawa
popeza samafuna kulima. Akapha nyama yambiri amasintha ndi chimanga kapena mtedza. Nyama ina
imagulitsidwa ndipo yotsala amachita ndiwo.

Ngakhale kuti zankhuli zidali kutapa kutaya pakhomo pa Naphiri, iye adali odandaula nthawi zonse
popeza ankalima yekha. Usiku wa tsiku lina Naphiri adaletsa mwamuna wake kuti asapite ku liwamba.
Adamulangiza kuti adzichita liwamba m’nyengo ya mwamvu akatha kulima ndi kukolola. Pingeni
sadalabadire izi konse.

Mwachizolowezi m’mawa wa tsiku lina, Pingenni adalawirira kupita kokasaka. Akulowa m’nkhalango
muja adaona mapazi a insa. Iye adadziwa kuti insayo ili pafupi ndipo adayamba kulondola mapaziwo.
Atangoyenda pang’ono mozungulira chulu chowirira adawona chiwande. Mosakhalitsa adamva
mtswatswa ndipo poyang’anitsitsa adaona kambuku akutuluka pa chulu mwaukali. Apatu Pingeni
adangoti phazi thandize. Adafika kumudzi akunjenjemera kwambiri ndi mantha. Kuchokera apo Pingeni
adaleka kusaka ndipo adayamba kulima molimbikira.

Tsopano yankhani mafunso otsatirawa.

a. Kodi nkhalango ya Maliwati idali kuti?

b. N’chifukwa chiyani nkhalango ya Maliwati idali yoopsa?

c. N’chifukwa chiyani Pingeni adali wokonda kusaka?

d. Fotokozani kufunika kochita liwamba nyengo ya mwamvu.

e. Fotokozani zinthu zitatu zomwe Pingeni adaona m’nkhalango muja.

f. N’chifukwa chiyani Naphiri amkadandaula nthawi zonse?

g. Perekani matanthauzo amawu otsatirawa:


(i) Kutapa kutaya
(ii) Phazi thandize
h. Pezani mawu m’nkhaniyi omwe ndi ofanana ndi awa:
(i) Gwape
(ii) Kunyozera
i. Perekani makhalidwe awiri a Pingeni.
j. Tchulani makhalidwe awiri a Pingeni omwe akutsimikizira kuti kuti adasintha.

k. Pezani mutu woyenera wankhaniyi.

GAWO C (10 MALIKISI)


4. Werengani kankhanika ndipo yankhani mafunso otsatirawo.

“Tikulandireni ophunzira nonse. Takumananso mchigawo chino choyamba mutakhala kutchuthi cha
masabata asanau ndi awiri. Tikumbutsane kuti malamulo pa sukulu pano sadasinthe. Ndikupempheni
kuti tikachoka pa malo ano, tikagwire ntchito m’malo athu kenako tikalowe mkalasi kuti tikayambe
kumphunzira.

Mafunso

(a) (i) Kodi ndi malonje anji omwe mwawerengawa?

(ii) Angayankhule malonjewa ndi ndani?

(iii) Ndi ndani amene akuyankhulidwa mmalonjewa?

(b) Fotokozani njira imodzi yopewera matenda atsopano a COVID – 19 pa sukulu yanu.

(c) Kodi ndani ali ndi udindo olangiza anthu m’mudzi?

5. Pangani ziganizo zomveka bwino ndi mawu.


a. Litsipa
b. Jeda
c. mbu
d. nkhuti
e. mayani
GAWO D (40 MALIKISI)

Zungulizani lembo lokhoza A, B, C kapena D m’mafunso otsatirawa.

Mafunso 6 mpaka 10: Sankhani mitundu ya mawu omwe atsekedwa mzere kunsi kwawo.

6. Ganizo lanu ndi lomveka. 9. Mbuzi yakuda ija yasowa.


a. Mlowammalo c. m’neni a. Mneni c. mfotokozi
b. Dzina d. mlumikizi b. Mlowammalo d. mlumikizi

7. Bambo chiswe amalemba zinthu mofatsa 10. Zake zidalipo ndipo.


a. Mfotokozi c. muonjezi a. Mlowammalo c. mfotokozi
b. Mneni d. dzina b. Mlumikizi d. muonjezi

Mafunso 11 mpaka 15 sankhani mitundu ya


8. Kalanga ine! Mbewu zonse zakokoloka.
nsinjiro za chiyankhulo zotsatirazi.
a. Mvekero c. mlowammalo
b. Mfotokozi d. mneni 11. Kodi mbuzi m’kasaka zimalowa.
a. Ntchedzero c. ndagi
b. Nseketso d. chifanifani b. Litsiro d. njala

12. Chidziwe umo mlamba ndi mmodzi. 23. Zonda


a. Chining’a c. mkuluwiko a. Chita chipongwe
b. Ndagi d. mzimbayitso b. Dana
c. Nyozana
13. Kuning’a pa mimba ngati mavu. d. Sankhana
a. Chining’a c. mzimbayitso
b. Mkuluwiko d. chilapi 24. Gule
a. Chamba c. malipenga
14. Wayabwidwa ndi chitedze. b. Usiwa d. dansi
a. Ndagi c. chining’a
b. Mkuluwiko d. ntchedzero 25. Lemera
a. Peza c. zonse mom’mo
15. Watchera kumwezi nkhanga zaona. b. Wirira d. khupuka
a. Ntchedzero c. mzimbayitso
b. Chining’a d. Mkuluwiko 26. Chilaso
a. Chijalo c. chibayo
Mafunso 16 mpaka 20: sankhani gulu la
b. Chipiko d. chipato
mayina omwe ali m’musimu ulimi.
Mafunso 27 mpaka 31: Sankhani nthawi ya
16. Ulimi
aneni omwe ali ndi mzere kunsi kwawo.
a. U – ma c. Li – ma
b. Mu – a d. Chi – zi 27. Tiyalenawo akusankha fodya.
a. Yamtsogolo
17. Kuyimba b. Yakawirikawiri
a. Li – ma c. ku + tsinde la mneni c. Yatsopano yopitirira
b. Mu – mi d. Chi – zi d. Yakale
18. Nkhosa
a. Ka – ti 28. Tonse timasewera mpira mmamawu.
b. Ku – pa – mu a. Yatsopano
c. Mu – a b. Yakale
d. I – zi c. Yamtsogolo
d. Yamtsogolo yakawirikawiri.
19. Malipande
a. U – ma c. Ka – ti 29. Iwo adzakhala atamanga nyumba yawo.
b. Chi – zi d. Li – ma a. Yamtsogolo yathayi
b. Yatsopano yopitirira
20. Kagalu c. Yamtsogolo yopitirira
a. Li – ma c. I – zi d. Yamtsogolo yakawirikawiri
b. Ka – ti d. Mu – a
30. Jumbe waba nkhuku.
Mafunso 21 mpaka 26: Sankhani mawu
a. Yakale c. yathayi
ofanana mmatanthauzo ndi omwe ali
b. Yatsopano d. yatsopano yathayi
mmusika.

21. Mphaka 31. Ine ndimkalemba bwino kale.


a. Mbuzi c. changa a. Yakale yopitilira
b. Chona d. kalulu b. Yakale yakawirikawiri
c. Yakale yathayi
22. Kalowam’malaya d. Yakale yathayi yopitilira
a. Nsabwe c. wakuba
Mafunso 32 mpaka 36: Sankhani ziganizo atsekedwa mzere kunsi kwawo mziganizo
zomwe zili ndi zizindikiro zamkalembedwe zotsatirazi.
zoyenera.
37. Abambo apita ku vepi
32. a. Kumunda c. kuntchito
a. Kodi, kam’matumbayu adabwera liti? b. Kumsika d. kumalonda
b. Kodi kammatumbayu adabwera liti. 38. Yohane wagwira mkazi wokongola.
c. Kodi kam’matumbayu? adabwera liti. a. Wakwatira c. wafunsira
d. Kodi Kammatumbayu adabwera liti? b. Wapeza d. wamenya

33. 39. Ife ndife anyamata ovaya.


a. Mayo Ndabaidwa ndi msomali. a. Ozitsata c. otsogola
b. Mayo! ndabaidwa ndi msomali. b. Owala d. owoneka bwino
c. Mayo! Ndabaidwa ndi msomali.
d. Mayo, ndabaidwa ndi msomali. 40. Iye wandigulira nsapato buleti.
a. Yatsopano c. yokongola
34. b. Yolimba d. yowala
a. Namoyo adati, “amenewo ndi maganizo
Mafunso 41 mpaka 45: Sankhani yankho
abwino”.
lomwe likupereka matanthauzo a mawu
b. Namoyo adati amenewo ndi maganizo
otsatirawa.
abwino.
c. Namoyo adati, amenewo ndi maganizo 41. Dzuwa
abwino. 1. Ludzu 2 chajira 3 chilala 4 nthaka
d. “Namoyo adati” amenewo ndi maganizo a. 3 ndi 4 c. 2 ndi 8
abwino. b. 1 ndi 3 d. 1 ndi 2

35. 42. Chipanda


a. Chifukwa cha njala adamaliza nsima 1. Chobaya 2 chiwalo chathupi 3
yonse. chomenya 4 cha mowa
b. Chifukwa, cha njala adamaliza nsima a. 1 ndi 2 c. 2 ndi 3
yonse. b. 3 ndi 4 d. 1 ndi 2
c. Chifukwa cha njala, adamaliza nsima
yonse. 43. Dziko
d. Chifukwa cha njala adamaliza, nsima 1. Manda 2 Banja 3 lokhalamo 4 chikwati
yonse. a. 1 ndi 3 c. 3 ndi 4
b. 2 ndi 3 d. 1, 3 ndi 4
36.
a. Ndamva kuti mwabwera ndi ndalama, 44. Chikulu
zovala ndi ziwiya. 1. Galeta 2 matenda 3 mkhate 4 dengu
b. Ndamva kuti mwabwera ndi ndalama a. 1 ndi 2 c. 3 ndi 4
zovala ndi ziwiya. b. 1 ndi 3 d. 2 ndi 4
c. Ndamva, kuti mwabwera ndi ndalama
zovala ndi ziwiya. 45. Kamba
d. Ndamva kuti mwabwera ndi ndalama 1. Chifukwa 2 kanyama 3. Nkhani 4
zovala ndi ziwiya. chakudya
a. 1 ndi 3 c. 3 ndi 4
Mafunso 37 mpaka 40: Pezani mawu omwe
b. 2 ndi 3 d. 2 ndi 4
alembedwa moyenera ku mawu omwe

MAFUNSO ATHERA PANO.


DZIPEREKE PRIVATE PRIMARY EXAMINATIONS BOARD
2023-2024 TERM THREE MID-TERM EXAMINATIONS
SITANDADE 7
CHICHEWA (MALIKISI 100)

GAWO A (MALIKISI 30)


Langizo: Yankhani funso limodzi lokha mwa mafunso ali m’munsimu. Sankhani
chimangirizo kapena kalata.
1. Lembani chimangirizo pa mutu KAPENA
uwu: MATENDA A KOLERA. 2. Lembani kalata kwa mnzanu
Mwa zina tsatani izi polemba: yomudziwitsa za khalidwe loyipa
Ndime yoyamba lomwe lafala pa sukulu yanu. Mwa
• Mmene munthu angatengere zina tsatani izi polemba:
matendawa Ndime yoyamba
• Zizindikiro zimene munthu • Cholinga cha kalata
amasonyeza akamadwala • Khalidwe loyipa lomwe likuchitika
matendawa • Chomwe chidayambitsa khalidwelo
• Zina mwa zinthu zimene anthu Ndime yachiwiri
angachite munthu akamadwala • Kutalika kwa nthawi yomwe
matendawa khalidwelo lakhala likuchitika
Ndime yachiwiri • Magulu a anthu omwe akuchita
• Fotokozani kuopsa kwa matendawa khalidwelo
• Njira zimene anthu angapange • Zomwe mukuchita pothetsa
popewa matendawa khalidwelo
Ndime yachitatu Ndime yachitatu
• Fotokozani zimene inuyo mwachita • Mmene khalidwelo lasokonezera
kuti m’mudzi mwanu kuti maphunziro anu.
matendawa asavute

Page 1 of 4
GAWO B (MALIKISI 20)
Kumvetsa nkhani
3. Werengani nkhaniyi ndipo muyankhe mafunso.

Mdera la mfumu Chinyama mudali mudzi wotchedwa Musakha. Derali lidali la mkaka ndi
uchi. Kummawa kwa derail kudali nyanja yaikulu komanso yokongola. M’nyanjayi mudali
nsomba za mitundu yosiyanasiyana monga chambo, mphuta, micheni, milamba ndi zina
zambiri. Anthu ambiri amayamika Leza kuti adawapatsa boma labwino losasowa kanthu.
Anthu a kwa Chinyama adali ogwirizana kwambiri motero chitukuko chidali ponseponse
monga mijigo, sukulu, zipatala, milatho ndi nyumba zamakono.

Chifukwa cha chidwi chomwe amaonetsa mabungwe ambiri amathandiza derail ndi mphatso
zosiyanasiyana. Anthu ambiri adali ndi thanzi ndi nyonga chifukwa amapeza zofuna zawo
mosavutika. Nkhani ya umband ndi umbava kwai wo idali nkhambakamwa chifukwa
padalibe adali pa mavuto woti ayambitse mchitidwe woipawu.
Mafunso
Page 2 of 4
a. Ndi dera liti lomwe kudali mudzi wa Musakha?

b. N’chifukwa chiyani anthu amderali amayamikira Leza?

c. Tchulani ntchito ziwiri zachitukuko zomwe zimachitika m’derali.

d. Perekani chining’a chomwe chagwiritsidwa ntchito m’nkhaniyi pofuna kunena kuti


derail losasowa kanthu.

e. Perekani matanthauzo amawu awa:


i. Thanzi
ii. Nyonga
iii. Nkhamba kamwa
iv. Leza
f. Kodi chomwe chidapangitsa kuti derali likhale ndi chitukuko ndi chiyani?

g. Kodi nyanja yaikulu idali mbali iti mderali?

h. Ndi chifukwa chiyani umbava ndi Umbanda idali nkhambakamwa?

i. Kodi nyanja yamderali idali yooneka bwanji?

j. Kodi a mabungwe amathandizaderali ndi chiyani?

k. Chitukuko cha mderali chimathandiza bwanji anthu?

GAWO C (MALIKISI 10)


4. Werengani kankhanika ndipo muyankhe mafunso otsatirawa (malikisi 5)

“Tsopano ndimulore kuti aloze yekha yemwe adampatsa chinjacho. Akatero timtengera
pena.”

Mafunso
i. Tchulani mtundu wamalonje omwe mwawerengawo.

ii. Kodi mawu oti “chinjacho” akutanthauzanji?

iii. Mukuganiza kuti angayankhule mawu amanewa ndi ndani?

iv. Tchulani mchitidwe umodzi omwe umalepheretsa atsikana kumaliza maphunziro awo.

v. Kodi ndalama zimene zimaperekedwa kwa sing’anga asanapite kokafuna mankhwala


zimatchedwa chiyani?

Page 3 of 4
Kupanga ziganizo
5. Pangani ziganizo zomveka bwino zomveka bwino ndi mawu awa. (malikisi 5)
i. Lingalira

ii. Khweza

iii. Du

iv. Mpukutu

v. Ija

GAWO D (MALIKISI 40)


Mafunso 6 mpaka 10: Tchulani mitundu ya mawu omwe atsekedwa mzere kunsi kwawo
m’ziganizo zotsatirazi
6. Ndatopa chifukwa ndaphunzira kwambiri.
7. Tinapita kwa achimwene dzulo.
8. Ogo! Ufa uja watayika.
9. Kondwa adagwa pansi kuti khu.
10.Eliza wavala diresi lobiliwira.

Mafunso 11 mpaka 15. Lembani magulu a mayina omwe atsekedwamzere kunsi kwawo.
11.Chimbudzi chawo chagumuka.
12. Kumudzi kuli ukwati.
13.Kamnyamata kavala malaya okongola.
14.Ana agula mzimbe.
15.M’khitchini muli utsi wambiri.

Mafunso 16 mpaka 19: Tchulani mayina omwe akusonyeza chachimuna cha mayina
atsekedwa mzere kunsi kwawo m’ziganizo zotsatirazi.
16.A Chidothi ndi chumba oyenera kumusula.
17.Dona wake adamuuza kuti alembe kalata.
18.Tonse tiyenera kumvera mfumukazi.
19.Mkwatibwi adali wosangalala kwambiri.

Mafunso 20 mpaka 22: Lembani matanthauzo azilapi/ndagi zotsatirazi:


20.Ndifera kubala.
21.Make mbuu, mwana mbuu.
22.Sesani pakhomo padutsa achimtali.

Mafunso 23 mpaka 25: Lembani mawu ofanana m’matanthauzo ndi mawu omwe atsekedwa
mzere kunsi kwawo.
23.Amayi apita kumsika kokagula chimungulu.
24.Iwo aphika nyemba zochuluka.
25.Dzulo tinadyera masamba a maungu.
Page 4 of 4

You might also like